Enanu we know already kuti mukudya za mcp watulukira ung'onoung'ono mwayamba kale kutsekula mimba jealousy down ufumu ubwerere kwaini ake ngati tikufuna Malawi asinthe apo bi kayaa...
@ChilekaMoyenda
Сағат бұрын
Boma ❤❤❤❤ tupele
@MorrisTsoka
8 минут бұрын
Ngati adzaphatikizane ndi MCP adzapita yekha waona kale ma supporter ake waakana kale achikangawa awa pamenepo aganize bwino kwambiri..
@bvulumedewickson62
54 минут бұрын
Ndale zaku Malawi ndizamchibanja ndipo zongomazungulira ndipakamwa ndikumalemeletsa mtundu umodzi modzi omwewo. A Malawi tatopa ndi mabodza tikufuna change ngati yomwe anabweretsa a Bambo ake A Tupele.
@DavidPhiri-o6w
20 минут бұрын
Don't go for alliance we want GNU
@happybinali4673
15 минут бұрын
I think this guy needs chance
@GrecianWyson
59 минут бұрын
Atupere akuthawathawa Nkhani ya MCP ndukuuzan akulu akulu uyuyu sindikumuona bwino mayakhidwe Ake Koma abambo Ake Mmmmm sanayakheso molondola Koma tiva. Akayesela Ku lowa Ku MCP ndukuuzan ndithu apitako okha chipani achisiya. Sirius
@ChifundoThomas
Сағат бұрын
Atupele you can't be a president on this country because yo are too young on compain
Atupele wadyadi ndalama za chakwela akilephela. Bwanji kuyankha pa funso la chakwela
@BandahLemos
42 минут бұрын
Tiuzeni zanzeru apaa osat munenazo ai amalawi simungawapusitse ai kuli 50 pls 1 ufuna unene chani plan yanu taiziwa inu ndi pp mufuna mugawe ma vote cholinga zipani zina zisawine muli ku MCP l know your plan
@senaherbo3714
36 минут бұрын
Achinyamata satatipusitse Ali ndi mcp ameneyu Why akupanga chibwibwi? ....that shows he is hiding something to us ..... Atupele sungaputse Amalawi chisadziwa anayaimbira mfiti manja Unfunse kalindo
@PeterRabson-z3w
13 минут бұрын
Musapange matama atupere apa inu ndichipani chani simugakhale pasogolo na ikakhala ya 50+1 bcz chipani chanu n chaching'ono
@simonpaul6567
25 минут бұрын
Guys speech ya UDF siyolimbisa mtima ai UDF tisazayivotere ukufuna MCP to come again in government I can see their plan
@EvanceWame-v7v
2 сағат бұрын
Awa utsogoleli mulibe thandizilani MCP poti ndalama mwatenga kale
@DavidPhiri-o6w
24 минут бұрын
Mbuzi abambo ako woyamba ananamiza kuti agulira sapato aliyese zilikuti?
@MushyNaliwa
2 сағат бұрын
Mmmm zamumtima nzawekha choona chili muntima mwawomo
Salary simuzalandila , iwe ndi Abambo ako tagwelani uko akuba inu... You are leopard you can't change your behavior... poorest education than ever during your Father time
Пікірлер: 107