Aaaaaa iwe ulibe ulesi kuzilowera kutenga malore ku mcp ko aaaaaaukuona ngati mizimu imeneyi igona owooooo ikusowesani mtenderetu
@AlexManuelMisomali-sv1vn
25 күн бұрын
😂😂😂😂 m'gwilidzano watha ?
@user-ln5hw7dn9g
25 күн бұрын
Dennis mlowa mmalo wa Chilima
@user-lz4kc5ob1t
25 күн бұрын
UTM yikhodza kupanga kamupeni siku limodzi ndkulowa mboma
@BrianZenengeya
20 күн бұрын
2025 boma
@raphaelbanda875
25 күн бұрын
Pls utm musatsogoze dyera ..let's join hands and fight we have sympathy vote....
@MarvinPeason
24 күн бұрын
I support it
@MaxwellSakwata-wb8ep
25 күн бұрын
UTM for ever
@GeorgePhiri-ub2of
25 күн бұрын
Koma utm madrama tikuonelani kumene mukathele ife pheeeeee ndi chakwela wathuyu 2025boma kale
@user-qp8kh2hj9o
25 күн бұрын
Aaaa kagwere ndi Chakwera wakoyo iwe mwana Wa anjoka iwe nde ukakhala kuti mfiti
@FanuelMaponda
25 күн бұрын
Uziwona nd nyau zakozo
@user-ml4bl2ll2g
25 күн бұрын
Kuvota ndi ufulu wathu sipafunika kuti munthu akhale ndi Cha unzika kuti akavote, please don't take Malawians for granted, don't block people from voting
@GloriaKaduya
25 күн бұрын
Kwambiri asatitengere ku dodo ngati ndife maliro anjoka ai it's our rights to vote
@chrissyyendayenda4650
25 күн бұрын
Skc my vote ❤
@user-xz3nz7dy1f
25 күн бұрын
Olo thawi ya yesu ayuda adazindikira kt yesu anali pulumutsi atamupha kale .... Ndiye azindikira kt skc anali pulumutsi wathu ndipo amakondedwa komaso ntendere alibe okuphao
Пікірлер: 80