Akuzakhala running met wa APM MUZANDISIMIKIZA IYI N MISSION mark my wards
@PharrohmagawaZimba230
Ай бұрын
100%
@PharrohmagawaZimba230
Ай бұрын
100%
@isaihmagani5697
Ай бұрын
Nde runningmate azayimira chipani chanji poti ku UTM azayimira Mary Chilima
@actuarialscience2283
Ай бұрын
He is our president at UTM. Wachoka kuchipinda kupita pa seating room. UTM and DPP we are one.
@hamischikalimba6626
Ай бұрын
Welcome to our beloved party UTM osaopa, osafooka osatopa SKC ndi ineyo ndi iweyo ndi ifeyo
@user-hm9nc7lz6e
Ай бұрын
Akabambe amafuna uprezdent ndiye mmene inangocitika ngodzi ya kuchikagawa achilima mkutisiya mumtima mwawo.amakondwa kuti atenga uprezdent ku utm akuluwa musavutike nawo asiyeni akaimire ku utm
@thokojames5231
Ай бұрын
Musaiwale naenso anali gulu lofuna kuba chipani la kondwani nankumwa ,komanso after kuionera patali kuti sangamake pa adad basino kuthawira ku UTM KUMENEKO MPATA AKAUUPEZA ayende bwino usazabwerenso ku dpp
@jeremiahmalikebu2393
Ай бұрын
Dalitso was a favourite wa adad, he is the only one amene adad amamukhulupilira kuti atha kumupanga endorse. Believe me, iyiyi ndi movie ma guys wa(adad ndi Kabambe) akudziwana.
@user-st6bt5vv9c
Ай бұрын
Mwana amalira ninkodzo wake asiyeni ayende bwino both him and others are not settled kutha kwamunthu kumeneko
@thokojames5231
Ай бұрын
Komano movie imenei zitengera kuti akupitako akakhaladi president
Musapusitsike inu izi ndiye amati ndale zenizeni akungofuna kutipusitsa awa ,iyi ndi plan yoti dpp yonse idakhalilana pansi kuti ipangidwe ndicholinga choti utm ija ijoyiniletu ku dpp ndiye kabambe watumidwa ngati nthumwi kuchokela ku dpp kulowa utm.woooo!
@yassinn5634
Ай бұрын
Pitani ku UTM.We want energetic leaders in UTM
@leonardmalirana7423
Ай бұрын
Pamene zafikapa sip
@user-nu1dj3jh7b
Ай бұрын
Njomba zimenezo kufuna kupusitsa a Malawi 😂, adakali ku dpp komweko koma akufuna apusise wanthu apite ku utm akatero akasankhidwa kukhala president wa utm kenako azapange n'gwirizano ndi DPP ndiye ku dppko azakhala VP wa peter akatero peter azachita resign ndiyekuti kabambe azasala nkukhala president wa DPP. Izi nzomwe amadananazo achina Nankhwa aja , peter waku Thyolo, kabambe waku thyolonso.akufuna azasiilane mpando anthuwa akuziwa chomwe akuchita
@user-gp10.10
Ай бұрын
Apa mwaganizo mozama bro,zitha kukhaladi chomcho
@user-qp8kh2hj9o
Ай бұрын
Aaaa palibe ubwino wake mnzeru za alliance ife a UTM tadzidziwa ndipo tikudzidziwa takula nazo mpaka taluza president wathu palibe angavotere izi mukunena iwalani
Apa nde akufunadi kuimaliza UTm cholinga akasakhidwe kudzakhala Vice president kuti UTM itheretu iyi ndi plan
@FarookStambuli
Ай бұрын
Welcome Mr kabambe to utm
@isaihmagani5697
Ай бұрын
Welcome to UTM monga ngati member chabe osati President
@paularason
Ай бұрын
Welcome to UTM Mr
@ChifundoChiwanda-ru3pg
Ай бұрын
Ngati akufuna kupita ku UTM apite koma tione kaye performance yake Ali ku reserve bank and also ku DPP. sometimes timakhala ndi anthu oti atha kugwila ntchito bwino dziko ndikutukuka koma amalephera chifukwa sapatsidwa mpaka bwinobwino or kuwagwiritsa ntchito mosiyana ndi mbali yomwe iwowo amayiziwa and atha kupanga deliver mosavutikira if they given the necessary resources. So I believe ngati anagwirako ntchito ngati nkulu wa reserve bank nzeru zilimo, he can be useful ku dziko lathu
@RobertLuka-wy9cl
Ай бұрын
Wayiwonera patali sangamake pa Apm
@isaihmagani5697
Ай бұрын
Osapusisika inu uyu ndi Cousin wa APM pachi bale chawo
@PatrickMtira
Ай бұрын
Mwapusa mr mukanangokhara komweko bwezi trem inayo akanakupatsani kuti mudzaimire km apa palibe mwachita
@robertkalima874
Ай бұрын
wachita bwino kusiya chipani cha kubanja
@JasonMailos
Ай бұрын
Muuzeni akalowe Ku MCP asati nyatsa
@AbdulrahimoMassamba
Ай бұрын
A UTM musanyadire,woteroyo ngwa dyera
@user-vx5kv8dz3d
Ай бұрын
Wachita bwino akalowe UTM . Vote yanga azaipeza
@user-ru1mm7bf4p
Ай бұрын
Wadabwitsa ndani munthu olo chipani alibe
@BrianJoe-z7u
Ай бұрын
Aaaaakabambe kabambe
@user-jj1zv2rs7f
Ай бұрын
Munalibe impact iliyonse mwainu yen Danish bwino
@user-kq6rp6hn7y
Ай бұрын
Welcome to UTM
@user-jj1zv2rs7f
Ай бұрын
Go well
@AndreaSignala-hk2yg
Ай бұрын
DPP 2025 boma muzakumbuka
@yassinn5634
Ай бұрын
Kabambe akuthawa chani ku DPP? Kapena Biden wa Malawi?
@amonfrancisautotune2073
Ай бұрын
Kkkkkkkl😂😂
@user-qp8kh2hj9o
Ай бұрын
Akuthawa chipani cha family watopa nacho
@ChrifordBiziel
Ай бұрын
Zakhara bwino chipan cha banja ichi
@eliaskachali-xn2ve
Ай бұрын
Pitani ku aford basi
@SaidiMbawa-st6bj
Ай бұрын
Ku Dpp usogoleri kulibeko koma dyela kukakamila udindo gogo imeneija osapasako mpata achinyamata
@DalitsoMatope
Ай бұрын
Achinyamata ngati inu alepheratu
@MzadziWanga
Ай бұрын
Chakwera wapasa ndani mpata?? Mesa nae wakakamira 😅
@DalitsoMatope
Ай бұрын
@@MzadziWangaakufuna amalizitse kudya misokho ya malawi
@SaidiMbawa-st6bj
Ай бұрын
@@DalitsoMatope zikugwilizana bwanji usogoleri ukufunika kwa Ana chakwela so ndi wachikulire bola awa not gogo ngati Peter kabambe kuti achoke kuli vuto kumeneko uzavomereza mochedwa
@GanizaniKamvazaana
Ай бұрын
Ali ndi tsoka ameneyo
@hamischikalimba6626
Ай бұрын
Peter Mutharika sangasiye mpando once voted into power unless death takes him. So l salute that decision Kabambe has made
@user-qp8kh2hj9o
Ай бұрын
Ndipo zoona Peter Munthalika sangasiye mpando wa chipani cha achimwene ake zoona
@user-nw6ie3xx8b
Ай бұрын
Prophet liyabunya analankhula za utm Zana kuti ayigula, liyabunya is not just a prophet like others no he is Elijah of our generation, love u prophet, bless me my name is Paul kheche mvuma
Catholic zoonadi ndi church ya pamalo pose koma mulibemo choonadi, like praying for the dead, Christmas, forgiving sins like God himself,kubatiza ana,ubatizonso wabodza,kuletsa kukwatila,kumafuna kupanga control boma pomwe church and state siziyenera kuphatikizana, kusintha sabata from surtuday to sunday,tsiku kumayamba usiku kuthanso usiku mmalo moti tsiku liziyamba kulowa kwa dzuwa kuthanso kulowa kwadzuwa ndi zina zambili bible likuti turukanimo mmenemo anthu anga babulo wagwa wagwa amayi wa a chigololo wa zonyasitsa za dziko ndipo mpingo umenewu uli ndi ana ake omwe amaitsatira zochita zakezo monga sunday keeping and all things that are out side the bible these practices are from pagan the chief of all paganism is the enemy of God called satan thanks for understanding ❤❤❤❤
Пікірлер: 68