Mukaona munthu akuti MCP my vote ameneyo ndi wa family ya chakwera mwina ndi ankolo ake kapena chakwera anakwatira pakwawo which means phindu la chakwera akuliwona ameneyo wachita zolozeka kwawoko
@macdonaldmunthali9895
Ай бұрын
Very wrong decision,the end of utm.chilima was the only leader with great vision and calmness, you can't make decision out of anger.
Njawala number one, kaluati number two be careful ndi anthu awiriwa ndi anthu oyipa mutima kwambiri We love utm kwambiri koma isakhale ya munthu
@doreenkaliati3166
Ай бұрын
Zoona zake anganidze mofasa sure ❤❤❤❤❤
@JaphetSakala-pq4fl
Ай бұрын
UTM motomoto osadandaula
@MosesNanchinga
Ай бұрын
Ma comment onsewa bwanji simukukamba za ndalama ai kma UTM sinalakwitse kuchoka ku alliance coz sanalandire ulemu uku ku MCP atizuza ndlmazo mukukanika kugulira mankhwala zipatala bwnj
@TonykalicheloKalichelo
Ай бұрын
Inu ngat mwin wake amafuna kusazika ndiye mukufuna omusatila atan
@lyiemax
Ай бұрын
Proper narration, big up guys ❤❤❤
@RegistermoseskashonKashon
Ай бұрын
Inu nde munabwela kudzauza amalawi tchutchutchu osat akapilikon enawa ongokamba zinthu zopanda kumutu
@user-rf4br1fv2z
Ай бұрын
Mwawathandiza ulemu
@DalitsoPhiri-sq5nl
Ай бұрын
Skc ankafuna kutchoka after kusalemekdza mgwirizano omwe unalipo ndiyeno kutchoka it's a good move komano to agree with ndikutenga mnthu kunja that's wrong indeed
@EdsonNjonjo
Ай бұрын
Munthu uyu akunena zoona
@AlliSaiti
Ай бұрын
Athu akuda ndife opanda nzeru
@MervinKandoje
Ай бұрын
You to be specific
@OsmanMasamba-ck4mo
Ай бұрын
Manganya iwetu wagulidwa ndichisilu chinzako
@FloraBanda-w7t
Ай бұрын
Koma selina 😂😂😂akut kod akabambe akulowela kut 😂😂😂😂
@user-ux9ik4zr5x
Ай бұрын
Probably the best program
@InnocentEdasi
Ай бұрын
Ndibwino kt atengane okhaokah
@StevieTaiza-r9j
Ай бұрын
Mulungu azikutete bro
@user-vm7iz6oz6r
Ай бұрын
Akumatibera zathu zomwezi zamisokho
@EstherManda-ex3bc
Ай бұрын
🤣🤣🤣🤣 nkhani zake
@Aqiec09
Ай бұрын
Yea that's very true and I see it ku utm utsogoleri unali wa chilima ena onsewa mavuto bola ku MCP komweko mudziwa bwanji mwina the death of chilima was planned with those who are on top blaming MCP for the death yets amafuna mpando wachilimawo why so early kutuluka mugwilizana without solid proof that is MCP guilty , ine unless pa social media muzabwerese real proof how you saw the killing happen that's when I will find them guilty
@ChiyembekezoPhiri-sv8nw
Ай бұрын
Njawala ndi kaliati mutiwonongera chipani chathu ndakwiya Nanu heavy kuno kuntheu mutisamale awirinu
@Ishriss1999
Ай бұрын
Ma prophet watu koma atilankhilitsa pambali mxiiiiew
@mzeewandembonyirongo2972
Ай бұрын
Gwende u have fairly advised
@user-lg6ym4hz3w
Ай бұрын
Kkk😂😂😂😂😂😂😂😂 anzanga afumu owuka
@SabinaNkhoma-sf7kz
Ай бұрын
Mmmmm km mcp yaonjeza,zot amalawi akuvutika sakuganizako
Nduna zomwe zikugawa ndalamazo akumatibera misonkho yathu yomweyi...ifetu maso athu tikuona ndipo tilankhula chaka cha m'ma chino....40million plus just for one meeting business yanji imene akupanga? Apapa zaonekeratu kuti andale amatibera pomwe anthu akufa ndi njala. Ambuye akukuonani ndithu
@innocentissah2636
Ай бұрын
Pamaliro wandale athamangitsidwe
@JasonMailos
Ай бұрын
😢😢😢😂 ozuka kumandao Eeeeee kusokonezatu kkkkkkk
@cynthiakananji1608
Ай бұрын
First to comment
@MasaukoNyirongo
Ай бұрын
😂😂😂😂😂😂😂 koma zinaz abale kkkkkkk kuthamangitsa masiket mudzi kkkk
@SamKaposa-i5c
Ай бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂Koma abale
@AdenaGuest-g4b
Ай бұрын
Kuwechetamwangajimbilambali
@AdenaGuest-g4b
Ай бұрын
Aaaaa Malawi
@ZioneMkangadzula
Ай бұрын
utm igawana zida zafikapa angonamizana
@chrisgremu740
Ай бұрын
MCP 🔥🔥🔥🔥
@IshmaelIbrahim-s8c
Ай бұрын
Pathako pako 😂
@ThomasShuga
Ай бұрын
Wabaya ase kkkkkk@@IshmaelIbrahim-s8c
@ThomasShuga
Ай бұрын
Iwe fisi eti 😢😮
@user-he4jv1sb1m
Ай бұрын
Mapazi ako nd mcp yomweyo
@MaryNyirenda-nq3mh
Ай бұрын
Njoka iwe fiti
@AdenaGuest-g4b
Ай бұрын
Umakwana
@PociahMack
Ай бұрын
Kma nkhani ya a pro andiseketsa bwanj😂😂
@PhiriChitani
Ай бұрын
Ndinu a Mcp chokani apa mukuyiwala kuti UTM idayamba yokha without mcp
@user-nj5vu8cd5l
Ай бұрын
Usi ndi munthu yimodzi yomwe mwini wa UTM
@SprianoJeke
Ай бұрын
Kugawa ndalama Koma ma servants ndee ka salary ka mmanja
@SprianoJeke
Ай бұрын
As government I think abalalika ndithu
@ChristopherKabanga
Ай бұрын
vuto amalawi timasapota vitsilu kali ndi ........
@user-gk4nu4xr8r
Ай бұрын
Of course
@GeorgePhiri-ub2of
Ай бұрын
akuononga chipani cha utm ndi mai kaliati ndi azao filex njawala anthu awawa ndithu amaliza chipani cha utm samalani
@RhodaBandah-sh1ir
Ай бұрын
Tafotokozani mmene akuwonongela ....
@MsondaBanda
Ай бұрын
Ntchindi mulije mu utm
@user-kj7hr2jf1l
Ай бұрын
Zowona utm yisatenge munthu wakunja
@atupelemposa4786
Ай бұрын
😂😂😂
@MayesoKulea-sh8xd
Ай бұрын
MCP ☑️
@YohaneMotison
Ай бұрын
😂😂😂😂😂😂
@PulayaKalaka
Ай бұрын
Mcp mooootooooooooo
@user-cb5gh9md4i
Ай бұрын
Kodi ntchentche zikutanipo pamibawapo
@officemoyenda-rj2hz
Ай бұрын
Si ntchentche
@SamKaposa-i5c
Ай бұрын
😂😂😂😂😂
@FloraBanda-w7t
Ай бұрын
😂😂😂😂esh I think ndi lens
@YamikanAbubakary-my4ie
Ай бұрын
Ambuye mulungu daritsani chipani cha mcp 🇲🇼❤️ 🙏🙏
@Extratremendouszeus
Ай бұрын
Ndiwe opembedza mafano Mulungu wa Abraham sangadalitse MCP...siwachisokonezo ngat Chakwera wakoyo...usamutchule Mulungu pachabe...ungaone tsoka
@user-px6kt8rx2p
Ай бұрын
Ukunama ukadakhumudwa mcp chiyembekezo cha Malawi ambiri
@robertkalima874
Ай бұрын
@@user-px6kt8rx2p MCP chipani chafuko
@SamKaposa-i5c
Ай бұрын
Usatchule dzina lamulungu wako pachabe chome iwe
@MosesNanchinga
Ай бұрын
Ma comment onsewa bwanji simukukamba za ndalama ai kma UTM sinalakwitse kuchoka ku alliance coz sanalandire ulemu uku ku MCP atizuza ndlmazo mukukanika kugulira mankhwala zipatala bwnj
@Extratremendouszeus
Ай бұрын
Abwenza ndalamazi...eni ake akutuwa kusowa sopo...akuoneka a fumbi lokha lokha km ena akuononga mosaopa Mulungu...ayi tiona posachedwapa....nafe tikudikira
Пікірлер: 100