I don't support any idea of making Alliances with Dpp because both Dpp and MCP is ruled by people of same ideology of the one party system. I think the good think UTM can do is to rebuild party with its new ideology but for the coming 10 years. It should have the long term goals by encouraging and promoting new ideas among youths who will be more voters in 2030 while expanding their presence in the parliament.
@PatKabiya-hy3vm
25 күн бұрын
Alimbikitsen a UTM Mr Kalindo... palibeso mavuto amene akumane nawo..bola alliance yathapo...let them keeping forward that's all..✊
@PhillipjuniorGogoda
22 күн бұрын
more fire DC🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@user-qn2nu4xs9i
26 күн бұрын
Easy...easy....tawaona kale...ticheza nawo ...zaozo sizitheka!😊😊😊😊😊..anthu ali maso
@EbenTechnologies-xq5op
26 күн бұрын
UTM, Aford, PP should merge their parties to defeat MCP
@chelseajackson3200
20 күн бұрын
JB is MCP.
@MarkManyowa
26 күн бұрын
For Presidency Born Kalimdo ☘️🇹🇿🔥🔥
@IyahMohyoh
26 күн бұрын
Ine si mzika ya Malawi, koma ndinkakhala zaka 13 mu dziko, ndipo ndidzahkalanso. Ndinkamuuza anthu poyambira chaka cha dzana kuti njira imodzi yokutithandiza kugonjetsa ndiye ndi yomweyi. UTM atengane ndi DPP, komwe a Chilima anachokera. Maso anga amanyowa ndikamameera zinkhani zikuchitika. Mlengi wathu atitsogolere mu nkhondoyi. Zikamatentha kumenya zitadzakoma kugonjetsa. Without confidence one and ones are twice defeated in this race of life(Marcus Garvey). Moto iyake basi. Kusengezeratu mwa kathithi. Love an peace. Best wishes 11 thousand km away from you my people. Ndimakunyadirani kwambiri❤❤❤
Koma kalindo anakonza ifetinkaona Kuti awa awa analindi cholinga because munthu amalandila malangizo aabwana ke Koma uyu Mmmm anati escariot uyu😂😂😂 aziona next step
@MirriamKambale
22 күн бұрын
Bon Kalindo alibe mbali that's one thing about him I like amangotulutsa mabvuto wambalizonse ndiku ng'alula iye wautali azabweranso ndiina. Mumisala yakeyi mulinso mfundozina zabwino andalenu tolanimo zothandizazo wamisalatu adaona nkhondo the dddd cccc 😂
@user-uv5rf4zt5q
23 күн бұрын
Federal system of government is the only way to go.
@AllySafali
23 күн бұрын
Mayine big man kuzatulukila ndikung'alula mwanyooo God bless u Mr kalindo
@joebrown1158
26 күн бұрын
To be honest Malawian the government is no longer existed there's no government to rule Malawi how is going to be the Parliament without the alliance of the government because that government was formed because of alliance
@IyahMohyoh
26 күн бұрын
Tsogolo lathu lowala ili mmanja wathu, Mlengi wathu atitsogolere . Kwacha dzukani, tulo ndi lokama, koma ufulu ndi mtendere ndi zithu za mtengo wa patali.
@user-lc3sw8iz2g
26 күн бұрын
A UTM ngati akufuna Congress igwe ndiye kuti agwile tchito ndi DPP. Chifukwa Second term ya MCP idzapanga zokuti UTM ithe.
@viennasamuel2976
25 күн бұрын
Ndipo zoonadi kungowamvetsa kuwawa a mcp atuluke
@isaihmagani5697
21 күн бұрын
Sunganene kuti DPP igwire ntchito ndi UTM
@LysonMtalika-tb6fk
23 күн бұрын
Honestly speaking from our beloved president, the Dddddd Cccccc!!!! 🔥🔥🔥
@williamsalexmbonga
22 күн бұрын
Nde mukufuna Dr Usi apange risign iwe ndi Mbuzi Winiko eti
@RickMahangano
21 күн бұрын
The mouth of the voice less, i@the rest of the followers, we like your updates,
@AubreyChiyaya-ty8ge
26 күн бұрын
Gwesani MCP please kaloweni ku DPP
@alexanderlipenga1330
25 күн бұрын
Ine phee kumastand no more recycled politicians be it UDF, MCP, AFORD, DPP, PP, PDP, UTM. We want achinyamata tilamule tokha. NRC for the prosperous Malawi
@RamadanShafisha
23 күн бұрын
Kalindo azimutsatila ndimbuli zizake
@lastonkandiyado4526
23 күн бұрын
Manganya ndiye yudasi sikailoti
@danielmsowoya9107
24 күн бұрын
Politics is a game that needs proper strategy. In politics there is no permanent enemy. In my personal opinion, it can be wise enough to gang with DPP if DPP can accept it. Otherwise united we stand divided we fall.
DPP Must change your bad behavior lets try Aford mix leaders don't forget mr Chihana please
@sanlakedickson6780
25 күн бұрын
booooon kalindoooooooo❤
@user-ro1pl7rv7z
24 күн бұрын
Pachibale pawo
@IsaacKulongwe-ol5mx
25 күн бұрын
Only madness in u kalindo
@franknyasulu7328
23 күн бұрын
The only way for utm is to unite with DPP afford and udf , ldont think among this for partys can make alliance with mcp , most malawians want the alliance of DPP utm afford and udf
Chimene chavuta ku malawi ndi ufiti ndi nsanje, akupaseni inu u president tiwone ngati mungakane
@amontchuwa6876
23 күн бұрын
Mr pule Bon kalindo
@EllinaBitto
24 күн бұрын
Ing¹alule basi❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@FlechaChipeta
19 күн бұрын
❤
@PeterMajamanda
23 күн бұрын
I know what is Ndale and how
@GiftMwaungulu
25 күн бұрын
alliance ai zakamika
@languitoneelias9972
23 күн бұрын
Mumalimbana ndi chilima presdent wa utm ali moyo mwamukambila zambili lero wamwalira walowa manganya mwayambanso kodi munakhala bwanji inu
@AubreyTrust
26 күн бұрын
Kuying,alula kweni kwin kkkkkkkk kom
@OwenWalter-nz7uo
24 күн бұрын
The DC
@anifoiuene6301
25 күн бұрын
Koma nzoona kuti abambo amenewa (chakwera) anali m busa ?? Nanga ndi m busa wanji uyu osanva chisoni ndi nkhosa zake zomwe
@lillynhlema9656
24 күн бұрын
He was a fake pastor....adakakhqla mbusa weniweni sinmbwezi atajoina ndale
@MadalitsoChinkhonyo
26 күн бұрын
Zimenezo nde ayi ku dpp tinachokako basi iwowo ngati akufuna abwele ku utm basi dpp inati khakaza ife sitiyifuna
@IyahMohyoh
26 күн бұрын
Mwerani mayi Mary Chilima analankula dzulo kuti siyani chidani za ku mbuyo.u kuti tigonjetse anthu oyipa. Koma kufunika nkumalungalira mwozama.
@viennasamuel2976
25 күн бұрын
Ndipo wandiyankhulila bwino Mary
@yahgoshen5815
25 күн бұрын
Now in Malawi it is just dramas
@AlexKaunda-ny2eg
25 күн бұрын
Manganya ndi fiti size anafupika dzose ndi dzelu dzomwe
@dalitsonjewa4868
26 күн бұрын
Wamisala uyu😮😮😮😮
@sanlakedickson6780
25 күн бұрын
iweyo ndamene uli wamisala
@user-wl4nd7ic1s
25 күн бұрын
Nyauuu iweee
@user-xt2gu9yt9q
25 күн бұрын
Trapesi ndi Tambo nde gwelo mavuto akumalawi athu oipa kwambili koma ayi mcp yaonjedza
@user-hm9nc7lz6e
26 күн бұрын
Zoona autm bwererani ku dpp ndi komwe munacokera
@hanifahmponda8711
26 күн бұрын
Aaa amalawi nsitilalola kuti voti opanda ma ID ansadzalembetse voti PAPO BOLANI IDZALEPHELEKE VOTE TIDZAWONE MENE AWONONGELA ZA ID IDZI OSUTSA WADZELU.ANGALOLE ABOMA KULENGEDZA KUTI OPANDA ID ASALEMBETSE VOTE OTSUSA NDIKUMVUMELA AKUDZIWA KUTI KUMWELA NDI KU POTO ANTHU AMBILI ALIBE MA ID DZIZAPANGA DZIWONETSELO ZA DZIKO LOSE KAYA AKUDALILA MAI YOLAMU TIDZAKOMANA KUTSEWU KOKO MCP IDZACHOKE NASI 2025 za ID ayiiiiiiiiiiiiiiiiiiiii TAKANA A MALAWI
UTM ikhale paokha basi. Masanzi akasanzidwa sadyedwanso. UTM isayang'ane 2025 koma izikonzekeretse za 2030. Migwirizanoyi ndiyakupha. Munthu sakhutitsidwa ndi ma udindo.
@Lee-lee-w1r
26 күн бұрын
Apa nde mwayankhuladi
@user-qp8kh2hj9o
26 күн бұрын
Zoona ndagwirizana nanu
@doreenkaliati3166
25 күн бұрын
Iwensotu ndi wabodza pena ndimkakukhulupilira koma apa ndiye ai mwataika kodi siwe umkati DPP siboma labwino umkasogolera mademo iwe lero ukuwaudza anthu kuti abwelere ku dpp uzi sizoona suuja umkanena kuti pita akupha malubino lero ukuti tiyeni ku dpp iwe ndakuona ndiwe nthera kuwiri sopano uyu musamamumvere bola UTM ipange gwilidzano ndi Aford osati dpp zaugalu basi or azaludze palibe vuto
@user-dm2fs6hf1b
24 күн бұрын
Ayi koma mcp is too much they failed what development has mcp done, devaluation fertilizer in dpp time was at 25000 now 95000 can't to see the different killing and intimidation. Sankakwanitsa zonse koma awawa angokwanitsa ma speech koma pa ground 0 pa 100
@vukanifracksonchinkonde7324
25 күн бұрын
Propaganda yanu yoti if a utm tipite ku Dpp zikuvutani.....iwe paja ndiwa Dpp.....we can't go back to egypt
Пікірлер: 74