The Dangerous Freedom Fighter of Malawi Nation, Kamulepo Kalua.. Our trust is on you Mr Kamulepo. Long live our freedom fighter
@BensonChilundu
19 күн бұрын
Mr.Kamulepo and this man Bon Kalindo,we don’t need Chakwera to proceed ruling this country up to November 2024.Please let’s organise tough strategies for him to step down.Bravo Kamulepo,Bravo Bon Kalindo
Good Messnge Mr kamulepo kaluwa, Chakwela you mast go watikwana
@TwalikiWisiki
18 күн бұрын
a veteran freedom fighter,, a comrade, last man standing
@user-eb2yo9bc9k
19 күн бұрын
Malawian majority is Malawian s not achewa, big up kamlepo no divisions in Malawi, Malawi is 1
@RobertLuka-wy9cl
19 күн бұрын
God bless mr kamulepo ❤❤❤❤
@user-pv9uk6sc3w
19 күн бұрын
A mr. Kamlepo Kalua munayamba kale kumenyela ufulu, ndipo sitilola a Malawi. Alephera achoke basi. A Malawi ndi okwiya kale ndi ulamuliro wa chakwera.
@samchibenene4458
19 күн бұрын
Mr unable kamulepo kaluwa you are a hero thanks dad for speaking the truth we know as anew generation
@PatrickNyasulu-kf6eq
19 күн бұрын
Munthu wankulu kuyankhula mosaopa ngat mene amayankhula nthawi ya kamuzu nde chakwera ndindaniso pano anthu anachenjera kusiyana ndi nthawi ya kamuzu
@SolomonNjolomole
19 күн бұрын
Powerful Mr kamlepo ❤❤❤
@user-uv5rf4zt5q
19 күн бұрын
To be honest Malawi is going backwards people voted for Tonse alliance for hoping better life but federal system of government is the only way enough is enough.
@kingsleyhopematchaya5184
19 күн бұрын
Koma sitima yayamba kudutsa ku area 50 inatha njanje
@chesterphiri7523
19 күн бұрын
A MCP aputa Munthu wolakwika.
@user-iu6mr5xu6r
19 күн бұрын
Nzeru zikacuruka Zina zimataika Cifukwa ninji munapanga zipani 9 kukhala Nonsa Alliance mukudziwa za ufulu wa zipani zambiri?
@matthewnyozani6596
18 күн бұрын
God bless you.
@MosesKalenge
19 күн бұрын
A kamlepo mulungu adzikudalitsani ❤🎉🎉🎉🎉
@LysonMtalika-tb6fk
19 күн бұрын
Well spoken loud and clear 🔥🔥🔥🔥
@AlexKaunda-ny2eg
19 күн бұрын
Mukusewela ndi kamlepo munthu amene amatha kupanga mabomba wanya chakwera
@vitumbikokamanga5869
19 күн бұрын
Am listening ❤❤❤❤❤❤go deeper ❤❤
@vincentmalaulo4046
19 күн бұрын
The message is clear
@FloridaMakwinja-eq2ek
19 күн бұрын
I love your speech bwana Kamlepo
@user-oh9bh1cl3b
19 күн бұрын
Good talking mr kamlepo
@user-dd1qq5xq1k
19 күн бұрын
More fire kamplepo❤❤
@MosesKalenge
19 күн бұрын
Good news Limpopo makwana💪💪
@MikeMerecah
19 күн бұрын
Comrate kamulepo kalua he is great man,
@ChrisjuZiyaya
19 күн бұрын
Atapezeka awiri atatu olimba mtima ngati Mr. Kaluwa ndithu things can change koma vuto ndi mantha amalawi😢😢😢
@MsondaBanda
19 күн бұрын
Federal system of government it's the best in Malawi, we wa development not to keep billions for Malawians in the pocket,
@IsaacMusa-py2jm
19 күн бұрын
Powerful 👊
@ettahchipeta4795
19 күн бұрын
Ekwendeni to Euthini anausiyizila pa T/A Mtwalo please wativwileko msewu wajimika chomene wula tikusuzgika pakuya kukaya ku Euthini mwee😢
@hamiltonsolomon3756
19 күн бұрын
Powerful 👍 👍 👍
@alfredyesaya9419
8 күн бұрын
Kamlepo adang'aza uyu ha is not the one I was listening in those good old years, he is mad now, shame
@user-nj4ob8jw6y
19 күн бұрын
Mr. Kamlepo Kaluwa, ndine Mponda kuno, ndidakali kuno ku Soweto, but a'm taking my pension next year, I will be meeting you next year. I think u remember, Japheth Nkhoma, Mr. Kanyongolo, Mr. Maseko all from Soweto
@PrescotMkhwema-gl4eq
19 күн бұрын
❤ the greatest chat
@miovekanola2780
19 күн бұрын
Kamulepo❤❤
@user-ln3zx6wo4w
19 күн бұрын
Tose tivota kuno
@innocentmusuli7380
19 күн бұрын
Take that word .they will not manage what is coming , i believe something big is coming i say it again something big is coming anyamata soon azuka ndipo it will be like Kenya 🇰🇪 anthu akatopa amatopa kuti topi kungotopa basi
@ZionekaMember
19 күн бұрын
Bravo Mr Kamlepo Kaluwa
@YakiKandeu
19 күн бұрын
Kandeu from south africa currently za ndengezi zisatidwe bohboh China chake sichilibwino
@GeorgeMjojo-ss4ob
19 күн бұрын
Following
@user-gg9hw4oj2v
19 күн бұрын
💪💪💪💪🔥🔥🔥
@user-oh9bh1cl3b
19 күн бұрын
Fight for Malawians mr tivote tonse opanda ma ID basi fire eee
@BrunoChakukuma
19 күн бұрын
Mwatikondwesha dada kaluwa u president ukumuyanani not galu uyo walipo watikomera chilima
@cynthiakananji1608
19 күн бұрын
A MALAWI TISALOLERE CHIPANI CHIMODZI CHOKUPHA ANTHU OSALAKWA. AMALAWI DZIKO LATHU SILACHIPANI CHIMODZI. AMALAWI TIYENI TILICHOSE DZIKO LATHU PA UMPHAWI WA MCP
@AbrahamTembo-z5k
14 күн бұрын
Tnauzidwa kt tizawuzidwa pakadutsa masiku 10, koma mpaka pano kuli ziiii!
@user-iu6mr5xu6r
19 күн бұрын
Inu a Nonse Alliance ndinu mwaba cilungamo CA a Malawi . Leromukamaphedwa, nokha mukudabwa! Mumanena kuti Peter wadaba vote za Chilima ndi za Chakwera. Za Atupere ndi ena Peter sanabe. Bwanji bwalo lamirandu linalola zipani 9 zikhale pamodzi? Tsono lero mukuti mukubwerera ku Cipani cimodzi? Pamenepa opusa ndani?
@ImanRashidi-so4oo
19 күн бұрын
✊✊✊✊✊l love your speech Kamulepo kaluwa
@ImanRashidi-so4oo
19 күн бұрын
Live from south Africa
@user-kw7wr4kq9w
19 күн бұрын
Mwayowoyako va zeruu mwahuno
@yassinn5634
19 күн бұрын
Akuti ntolakhani , osadziwa kuti CENTRAL GOVERNMENT OR FEDERAL GOVERNMENT ndichyani kukhuta NAPWIRI basi
@abwinoamatani4921
19 күн бұрын
Bola MCP isamuphe kamlepo. Anthu akupha awa. Mulungu chonde apengetseni misala a MCP
@isabelmartin7567
19 күн бұрын
Inu wakwanatu chakwela 😢😢😢
@KunyengaMoyo
19 күн бұрын
Ngt zili zomagendanazo muwaudze asayerekedze kufika ku southern region azaona nyekhwe
Bvuto ndi mcp administration umbuli wachuluka from the president down the line mbuli zokha zokha.
@JamesMaduka-wk8xi
20 күн бұрын
Strong speech mr kamlepo ambuye akutetezen bwana
@ThomasMlowoka
18 күн бұрын
Chilungamo
@user-jl6sq3ph1b
19 күн бұрын
Ofunika kwasumila amenewo a mcp
@melanin7770
18 күн бұрын
Let's violence now tawonelera nyasi nthawi yaitari
@ThokozaniMaulana-oi5hz
19 күн бұрын
Mmm but this chipani mcp mmmm not good
@user-co3wr3rn4h
19 күн бұрын
Kamulepo munthu mulala chomene
@eliaskachali-xn2ve
19 күн бұрын
Chakwera pa thako pako kwizako Kuno Ku muponto Yai .kutikomera mubaliwinthu Yai
@cynthiakananji1608
19 күн бұрын
Ndamene anayambisa democracy mmalawi. Simunthu wamba uyu. Ali ndi history
@HusseinMadani-k6f
19 күн бұрын
Zidze mzatonse
@user-zp3fb7el4z
19 күн бұрын
Mumanena chilungamo
@TwalikiWisiki
18 күн бұрын
Mcp yapalamula chitedze,,, when you pray for the rain deal with the mad too,, Chakwera umva madzi chaka chino ine Mulungu anandiyankhula momveka bwino kuti akuvupula kowopsya,uyaluka,, ngati ungathe umupatse makobili Mulunguyo tiwone, my God is exposing you this year you are finished,, awa ma prophet mwawapatsa ndalamawa akukunamizani ask me i will tell you what the Mighty Lord God said,, your judgement has just begun enjoy it
@sparkdymon3429
19 күн бұрын
Achikule munthu wazeru
@phillipstamaley7901
19 күн бұрын
Koma ndiye za mowadi zaziiiiii 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
@user-ri2vi2fd5v
19 күн бұрын
Tiye uko mwana wa mcp iwe kupusa kwako
@FosterChilumba
19 күн бұрын
IQ zero
@CatherineMbela
19 күн бұрын
Pita kanyele uko mwana wa nyau iwe
@MaryNyirenda-nq3mh
19 күн бұрын
Ngat manyi akugwiran kanyelereni musatinunkhise apa iya
@ChristopherKawilam
19 күн бұрын
Galu wachabe chabe
@user-vm7iz6oz6r
19 күн бұрын
2025 tikubwera komweko ife usilu ayi
@augustinechibbalazi8897
19 күн бұрын
Let's learn from South Africa what H E Ramaphosa had done t o bring unity and patriotism bent on his genuine philanthropy. Long-live!
@omarduwa3441
19 күн бұрын
Mcp she is not going anywhere
@ChisomoJinard
19 күн бұрын
😂😂😂😂 She is?
@HafsaAbwanali
19 күн бұрын
Chizungu cha mcp chimenecho kutathauza kuti onse ndi akazi wokhaokha Aku mcp ko 😂😂😂
@chachaamoah3592
19 күн бұрын
Lol😂😂😂
@spargomw
19 күн бұрын
Chizungu chaku gule😂😂😂😂
@MaryNyirenda-nq3mh
19 күн бұрын
Aweeeeee 😂😂
@ChimwemweKondowe-nj4lx
19 күн бұрын
Once an eagle always an eagle. We believe in you the real freedom fighter legend Kamulepo Kaluwa. We're going to vote without their stupid ID'S protocol
Пікірлер: 88