Alemba mmadzi amenewo olo akamapereka R2000 ifekuno ku Johannesburg sitingachite za kanunduzo. Azibale athu kumalawiko akuvutika kaamba ka boma lonunkha mcp
@HamanjaManyela
3 ай бұрын
Ndipo tikumva pain heavy
@vincentbarnes5872
3 ай бұрын
DPP sikuti inalinso ya bwino mulakwisa kwabasi. Utsogoleri wa DPP kapena MCP sitikuufuna ata pang’ono koma utsogoleri wa masomphenya a Dr Saulos Klaus Chilima
@AbrahamTembo-z5k
3 ай бұрын
You are one of the wise, just & intelligent people.
@HafsaAbwanali
3 ай бұрын
Uthengau upite kwa brother nthanyiwa auze boma la ku South Africa ko kuti dziko lawomo mwalowa zifwamba zochokera Ku malawi zabwera ndiupandu. Nde muziwauza madera. Omwe Ali azifwambawo apolice awangire akaponye chakulinderako azikalima masamba tizigula mashop mu asazatulukenso chifukwa akutengela phamvu kumanja powaona kupusa eni dziko nde anthanyiwa musankhale nchisoni ndi crocodile pple agwidwe basi komweko uthengau ugwirisireni ntchito kuti akamangidwa ena atengereppo phunziro
@HamanjaManyela
3 ай бұрын
Ndipo azikalimadi masamba kunoko asabwele
@ThompsonMakwakwa
2 ай бұрын
Awomberedwako chabe kuno!! Asamaletu other wise apita opanda moyo!!
AWAWA GUYS AKANGOFIKA MU JONZ MUNO AKAMABWERERA ABWERERE ATASINZINA , ASABWERERE AMOYO IFE TAGWIRIZANA NDI MA ETA TIKANGOWAPEZA TIKUWAVEKA MA TAYALA NKUOTCHA TIKANENA KU POLICE KUTI NDI ZIGAWENGA ZACHOKA KU MALAWI KUFUNA KUDZASOKONEZA DZIKO LINO, ASIYENI A BWERE TIKUMANA KONKUNO
@HamanjaManyela
3 ай бұрын
Tanguwawombela komweko afele komweko akuwononga ndalama za amalawi
@RitaKainga
2 ай бұрын
Tell them Comrade
@LouisChipanda-ux9dz
3 ай бұрын
Akunama amenewo tikangowadziwa akumana ndi ma tsotsi kunoku
@DysonNakhaphe-bo4dl
3 ай бұрын
Man mukutiyimilila and tikudziwa zambili kuzela mwa inu pitilizani
@AbudulJohn
3 ай бұрын
Anthu awa asatidanitse amphawi ife ndi dziko la south Africa mu south Africa ndikumene tikupezelako thandizo lathu tikumakwanisa kusamalila makolo ndi ana kumamiziku ndiye inu aboma chepesani za chibwanazo muzipanga ku mudzi Koko kuno ayi tikupondani tikakuziwa tikufinyani ndithu akunkuyu samalani chifukwa mwatulusa maso ndi chipani chanu mutha kufa ngati nkhandwe wokuba nkhuku musamale koma
Пікірлер: 29