It's not a good idea to make Mai Chilima leader of UTM. There's time. Meanwhile let her follow her career to the top.
@doreenkaliati3166
16 күн бұрын
Ndinaganidza izi tsiku limene Achilima anatisiya kuti Marry ngati amamukonda mwamuna wake kuchokera pansi pa mtima akuyenera kuimira u President now am so happy to hear that Osatopa osatopa Mary Ambuye akutsogolerani mu zonse chifukwa chipanichi mukapatsa munthu wina ndithu kutha kukhala komweko chikadzawina azatsintha zina Ndiye Ife sitikufuna kutichipani Cha UTM chinthe chonse Mah musafooke maso patsogolo❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@user-qp8kh2hj9o
16 күн бұрын
🙏Zoona zake ife tikufuna chipani chisathe compaign anapanga kale chilima timangiodkira tsku
@SamJalie
16 күн бұрын
This woman is gonna rise
@user-re7fo3be2z
16 күн бұрын
It's not good idea at all because we all know that there is vise president of UTM, that person he is the one who suppose to be incharge despite everything.
@WisdomMaseko-fi5sv
16 күн бұрын
Mai Mary mukane. Anthu asakuikeni Mau mkamwa
@AminahMussah
16 күн бұрын
ndipo bola asamale ana awo asaluzenso Mai wawo ayii
@kingsleymsampha2260
16 күн бұрын
Mary has got a capacity to govern but only if she is willing. Azibambo ena akupangaso dyera heavy atha kuphetsa chipanichitu oooooh....
@Namphuno
14 күн бұрын
Malangizo aulele,, mai chilima osayelekeza kulowa ndale,,ndale zimapha pitilizani zina zomwe mumapanga and live longer,,anthu akukukopani lerowa mawa atayiwala zonse azakutembunukilani kuti simunachitepo ndale muzaononga dzina lanu ndikuchosa ulemu onse wa inu komanso malemu,, osayesa.
@paulinekayuni1621
14 күн бұрын
Munthu analowa kale ndale nde mukuti asayerekeze kulowa bwanjiso.😅 Komaso mukati ndale zimapha kodi ose atati aziopa chonchco zingakhale bwa. Aliyese azafa even amene amapha anzawo. Ndipo zimenezo ndizomwe mwina atha kulimba nazo mtima kuti ngati mamuna wake anafa iye aoperanji
Mayi Chilima I believe she's not a politician,Kalindo bwanji?
@BillyMhone-jp3kn
16 күн бұрын
Tiyeni uko ndi Kalindo We need chilima legacy And Mai Mary chilima She was closest to skc she is only one can take utm
@wilisonbornface4282
16 күн бұрын
Live from SA cape town muzen kaliyati Mary akurila plz
@chrisboyce2
16 күн бұрын
Fredokiss president wa UTM ndipo SKC Forever in Our Hearts ❤
@MathewsNyate-y9g
16 күн бұрын
Kuwafusa kaye ali ready kutero,bcz kupanga run chipani ndi ndalama
@nathannbanda3345
16 күн бұрын
Alowepo Akweni
@SildaKatundu
16 күн бұрын
Kufuna kumuphetsanso eti,mulibe chisoni guys ee
@BillyMhone-jp3kn
16 күн бұрын
Kufa tose tizafa we need her now to take this party
@samchibenene4458
16 күн бұрын
Maganizo anga ndikuona kuti asankhe wina osati Mary ndare zotani zimenedzi munthu akayambisa chipani basi akamwarila or retirement chizikhara cha family aaaa amalawi this is another generation let's change gyz
@mosesnyirenda5010
10 күн бұрын
This a great idea
@LiamTennessee
16 күн бұрын
A kalindo ndi amene angatsogolele bwino UTM,, Ali ndi masomphenya ,munthu okonda dziko ndi anthu ake,,
@SamJalie
16 күн бұрын
Kalindo is illiterate
@inessmsiyambiri8517
16 күн бұрын
Kalindo anasiya ndale
@user-qp8kh2hj9o
16 күн бұрын
Kalindo azitani ku UTM mumasowa zoyankhula eti??
@leahkasiwa5033
16 күн бұрын
Kaliat ukhale iweyo bwanji osogolera UTM mary akadali kulira mwamuna wake please napapata
@BillyMhone-jp3kn
16 күн бұрын
We need Mai Mary Chilima must take over
@doreenkaliati3166
16 күн бұрын
Marry saphedwa mu dzina la Yesu ndipo satana achita manyanzi No matter kuti ndi banja koma tikupanga izi chifukwa mwamuna wake wamfa imfa yowawa zinakhala ali moyo Saulosi Chilima zinali zosatheka kusiilira mkazi wake mpandowu anthu inu kumaganidza pena MCP ikufuna chipanichi chithe kungoikapo munthu chisawawa akachifulitsa ku MCP aime Marry kuti chakwera achite manyanzi kuti ndinachitanji pompha Chilima uja?
@HellenNyambose
16 күн бұрын
Let's people choose their leader freely
@andrewchiusiwa3487
16 күн бұрын
❤❤❤
@asiyatujuma5507
16 күн бұрын
❤❤❤❤😊
@user-es4jt6ds8m
16 күн бұрын
Zoona mary aimepo ena achigulitsapo Chipani pliz osagulitsa
@isaihmagani5697
16 күн бұрын
Maganizo anga ndamenewo since day one SKC atatisiya, mmene nduonera mu UTM atsogoleri omwe angapitise UTM patsogolo ndi Mayi Chilima kapena Che Kaliati apo ayi atenga wakunja ngati achina Dalitso Mpinganjira or Kabambe ndekuti chikhara cha mphamvu nkuzawinaso
@user-gg9hw4oj2v
16 күн бұрын
❤❤
@KondwanKafuratira
13 күн бұрын
Shaa!!
@TiyanjaneMkwate-we8gu
16 күн бұрын
Bola Mayi Kaliat.
@shayrafernandeslatif9556
16 күн бұрын
Bwanji osayika mayi kaliyati
@williamsalexmbonga
12 күн бұрын
Osaikapo Uncle ake a Chilima yo bwanji kuti zimveke bwino
@AleksaWilliams-qc6cn
13 күн бұрын
Mmmmh musiyeni Mary pls,sakhani ena
@TaweniChavulaKamwendo
16 күн бұрын
Eeee 😳
@MalawiRiddles
16 күн бұрын
Mom Patricia kaliyati can do that
@LimbikaniKadzongwe
15 күн бұрын
It's possible to do that ,is a right person to fill the position let her to be....
@user-xo8ms5wh2s
14 күн бұрын
Amai chonde zisakuchedwetseni izi tapangani zosamala ana anu osati iziii mama chonde ndizopanda phindu iziii
@AlexKaunda-ny2eg
16 күн бұрын
😢 😢😢 guy's give madam chilima chance she can make it dont choose manganya his Judah's
Wachiwili wa malemu a Chilima ku chipani cha UTM amene ali Manganya anatuluka kalekale mu chipani cha UTM analowa malawi congress party. ndiye nkhani ya maudindo a ku UTM Manganya zisamukhudze ai chifukwa iyeyu ndi mpeni wa nsengwa wakuthwa konse konse. Madam Mary Chilima go ahead. inuyo a UTM musanvele maganizo a wanthu amene ali kunja kwa chipani chanu
@TheLeezo
16 күн бұрын
Noooo,leave her alone and let her grieve her husband bwino bwino. N I don't think politics is her thing. Akweni bwanji? That woman is a firecracker,she can make it.
Ulendodi wa chipan ndumenewu,kuganiza kwabwanji uku.?
@masakaunga4099
16 күн бұрын
Mary akudwala
@edsonnyasulu5394
16 күн бұрын
Koma vice wake akhale Denice thandwe mufana wa nzeru ku mzuzu
@LottiAffati
16 күн бұрын
angozosiya zimenezo mamuna wake uja anali katundu olemera, mapeto ake Mary amuphanso and poti ndiwamkazi nde azamupezerera heavy
@user-jl6tr9wv3h
16 күн бұрын
It's too early give her time to mourn her husband
@christophermtonga8535
16 күн бұрын
Take note that UTM is not a family party like Dpp, Udf and Aford
@Eric-gb9ms
16 күн бұрын
Who are you yourself talking this nonsense
@christophermtonga8535
16 күн бұрын
@@Eric-gb9ms I am a proud Malawian citizen exercising my right to share my views on the political landscape of my country, and you?.
@Shadreckdingiswayo
16 күн бұрын
Kodi Mayiwa atawina koma akuziwa zoti president sayenda opanda mamuna nde mufuna kunena kuti akwatira popano palibe chikondi akaimira alire bwino bwino mamuna wake apo bii anali kale ndi chibwedzi cha nseli
@RobertLuka-wy9cl
16 күн бұрын
Mukapanda kuzatenga bwino utm itha
@BillyMhone-jp3kn
16 күн бұрын
Never and never Mai Mary will carry her husband legacy
@user-si7po9sd5i
16 күн бұрын
Komatu ofunika amaiwa asamale.
@BrightonKamwendo-db1ci
16 күн бұрын
Maganizo anga ndimaona ku UTM kulibe munthu yemwe Ali ndichuma chomasuka ngati momwe analiri chilima ambili manja awo ndiouma paichi chipani sichinga ime Sono ngati Pali maganizo amarry chilima kuti asogolere tiyeni tipenphere kuti akhare iwoo pachifukwa ndipo UTM sizatha ngati zitatelo koma mukasankha mosaganiza UTM yantha basi chipanitu ndi dalama ndiye muone bwino anatisokoneza pamene paja ine ngati sapota wa UTM ndatelo
@HaroonMaundala-lg5lg
16 күн бұрын
Excellent mwalankhula bwino komaso moveka kwabasi. Ine ndine wa DPP koma fundo yanuyi ndagwilizana nayo. Uku nde kuphunzisana muchowonadi. Chipanichi akachitengela mosalongosoka chatha. Chifukwa chaka adatiphela chilima cholinga chake ndikupha chipanichiso.
@doreenkaliati3166
16 күн бұрын
Amen amen Dear
@user-co6sc8om5n
16 күн бұрын
Bola kaliati osati marry Mmmm
@joanaKachiwaya
16 күн бұрын
Musatibalalitse Mary yo ndiokwanira
@MaryMlomba
16 күн бұрын
Izi ndiye za ziii malawi mwayamba kuitenga ngati dziko lotseweletsa
@doreenkaliati3166
16 күн бұрын
Inu Inu VC wake uti Manganya asakupusitseni si wa UTM uyu anakakhala ndi wa UTM sanakora kukhala Vice chifukwa Chilima wafa imfa yowawa inu uyu ndi MCP mkuthekanso plan yopha Chilima inachokera kwa Maiko usi cholinga akhalepo Iyeyo musamale nae maiko Usi
@GraceZumazuma
16 күн бұрын
Mary alire mamuna wake bwanji sankhani wina
@user-pn6py6rf6k
7 күн бұрын
Za family Kodi?
@SolokingChimzy-yt7dj
16 күн бұрын
Kkkkkkkkk Koma mau a Mulungu ndiowona sure..Dziko linachita khungu anthu lelo sakudziwa chomwe akupanga
Zipani za mabanja kkkkkkk koma Ku Malawi anaza tiye nazoni
@petertaulo8014
16 күн бұрын
Kuima kwa Madam Chilima ndifundo yabwino, pali anthu ena ali ndi ma plan ogulitsa Chipani kwa Ng'ona za mabango!
@VincentNyabanga-dw9uj
4 күн бұрын
Marry chikuni hi
@VincentNyabanga-dw9uj
4 күн бұрын
Marry chilima hy
@WanangwaMfune
16 күн бұрын
Zama banja izi asiyeni.
@PeterThomas-o9k
10 күн бұрын
Yoooohh Haybo she still crying his Husband she can't be leader that is people talking lie things
@Bonisiwentamo
16 күн бұрын
Koma koposa akhale wina mayi chilima ayi kuganiza kwanga chifukwa panopa Ali ndimaganizo ambili
@RuthChilobwe
16 күн бұрын
Even Patricia must not contest..Civil service suffered too much when Madam Joyce Banda was rolling Malawi .she hated civil servants and she grossly stole Malawi funds in her cash gate. So Malawi don't need women to be rulers OK notre women them are become so proud and pompous.. mpaka ife ma civil servants tinawapangirq mademo. Nkuwaika mbokosi ngqti amwalira.kkkk
@RuthChilobwe
16 күн бұрын
Ruling. Noy roling
@Lee-lee-w1r
16 күн бұрын
Exactly. As a female I agree
@SeanMatora
16 күн бұрын
Izizi ndi zomwe zikufunika Mary atenge mpando bas....❤
@user-re7fo3be2z
16 күн бұрын
It's not good idea to be honest
@DKMWALE-ew3lp
16 күн бұрын
Pambuyo panu madam
@user-lc3sw8iz2g
16 күн бұрын
Kwesi Msusa ndiye okuti atenge chipani cha Nzake Saulosi.
@Charlesnamalaka-uw6ug
16 күн бұрын
Yakhwesi ndaivotera,maiyu amusiye kaye
@edsonnyasulu5394
16 күн бұрын
Vice azakhale Denice mahata
@stalickkafera3454
16 күн бұрын
😂😂😂😂 komatu ma guys mpaka UTM mukufuna apatse WINIKO Za drama eti
@BlessingsTembenu
15 күн бұрын
Mery alibwino Kwa omwe timakonda chipanichi,komano atati wawina zizamupanga force kukwatila mwina asakufuna pomwe akulilabe mamuna wake coz sitikudziwa kuti inye mwini anayika nthawi yayitalibwanji kuti adzakhale pabanja.
@davidbulla5128
16 күн бұрын
💯 correct
@AlihIbrahim-s7v
16 күн бұрын
Incorrect
@GiftMwaungulu
15 күн бұрын
mufuna akwatiwexo pompano
@giftedmshan6779
16 күн бұрын
Mary tikufuna azawine 2025 azatifufuzile malilo a chilima
@SamJalie
16 күн бұрын
Manganya kagwere uko
@user-hl3st3cc4v
16 күн бұрын
Iwe zibambo wandemvu zako ukuti chipani Cha banja ndekuyakhula kwabwanji kumeneko tazikhalani ndi zeru poyakhula ngati zibambo siyeni mery ayime
@HaroonMaundala-lg5lg
16 күн бұрын
Aaaaaaa brother ndikuyankhani ponkhapo. Kumankhala ndikuganiza komaso muliganizile banjali. Palibe cha zelu mayi chilima kutenga mpando wa amuna awo. Mkaziyu adakali pa ululu kulila kulilila amunache. Ife athu akwathu ndikungosonkhezela. Ngati akwanisa kumupha chilima uja awawa nde chizimu. Asiyileni chuma chomwe awasiyila amuna awochi kuti chisasokonekeleyi. Samalilani moyo wa mayiwa.
@CyprianoSandalamu
16 күн бұрын
Mai Chilima musiyeni alire maliro amuna so,enanu kuthamanila kulakhula zosaveka,ngati Ali ndichuma maiwa asiyeni athandize ana ao osati muwasokonekeze mdzina loti aimilre muzidzawadyera bwino,sibwino siyeni alire Kaye maliro.
Пікірлер: 148