Ndiye MCP tikuidziwa ife ndimeneyo ndale zake ndi zakupha
@BrownMainje-sh7hj
28 күн бұрын
Shame on MCP
@augustMag
28 күн бұрын
Kwa APM yekhayo ndiye sangamukwanise dinner and dance ndi imeneyo koma Peter Muthalika yekhayo ku dinnerko Peter Muthalika akudziwa zokachita ifa ya Bingu Muthalika ndi ifa za anthu padege ukumupasa phunziro Peter amandisangalasa ndi omvera malangizo awanthu ngati Inu Amtanyiwa ndi Bakili Muluzi TV 🔥
@miketholiwa1762
27 күн бұрын
Asamale kwambiribe koma
@user-ky4ce9gb6j
27 күн бұрын
Eti
@user-ky4ce9gb6j
19 күн бұрын
@@augustMag ndipo kwambiri tu mmm
@AiameAdamo-su1nt
28 күн бұрын
I'm here following you step by step each and everyday.
@MayamikoBanda-jh8bn
28 күн бұрын
I love the way momwe mumachenjeza Malawi kwa zigawenga . Ndiye nimamutsatilani kwambiri pa KZitem Kono ku Zambia
@MaggieMujuma
28 күн бұрын
Eeeee mayo ndalama yanga ine Peter munthalika iwe ndi Wilson msemanjira iwe anthu okuba inu
Mwachita bwino Comrade mtanyiwa Tili nawenawe sitingakutaye
@user-dn3gp6yi4y
28 күн бұрын
Kumeneko ndiye ku mafelano kuja sopano koma anthu awa akuti bwanji ndi dziko lathu cholinga chawo ndi chani? Komaso asilikali athu angoti ziiiii kumangowonelela dziko likuwinengeka koma zoti abale awo ndi makolo awo ku mamamidziku akuvutika iwowo sakuziwa kodi? Nanga chomwe akumakhalila chete ndi chani ? Chakwela kwake kwatha ife tikufuna mtendele mu dziko musakomedwe ndi ndalama komaso omwe akudya ndalama za magazizi si asikali onse pali omwe akumadya enanu dzukani kutha ndi boma lopusali lakupha la mabodza komaso pa katangale azathu aku mangochi tetedzani PM kumeneko akaziwika anthuwo apondeni or kuwapha kumene np afela zintchito zawo
@VeronicaChirwa-ct4os
28 күн бұрын
Asilikali a Malawi amawoneka kuti ndi opepera safuna kuthandiza Zika za Malawi akowopa kuyimbira anthu akulemekeza zigawenga zi Achina Chakwera
@AlexMbewe-p7y
28 күн бұрын
NDIPO SIZITHEKA AYI MULUNGU ALI KOMWEKO AMENEUJA SANGAKWANISE CHAKWERA KWAKE KWATHA NDIPO ALI NDI THAWI YOCHEPA MULUNGU AMULANGA ANANGOKHALA BUSA KOMA NDICHIGAWENGA CHACHABECHABE BUT I BELIEVE GOD IS THERE TO PROTECT PETER WA MUTHALIKA
@macdonaldkorea2928
28 күн бұрын
Or nkhope ya Chakwerayo ikuchitakuonetsa kut ndinkhandwe yoopsa....asapotilidze.konse aidya malawi yonse
@StelliaSangaya
24 күн бұрын
Zoonad
@ephraimphalawala4720
28 күн бұрын
In Jesus name, God protect APM
@PeterJames-i8y
28 күн бұрын
Mulungu amene anapulumutsa shadrec ,Mishec ndi abitinego kuphatikiza Daniel mudzenje lamikango apulumutsenso azitsogoleri amene atsalawa. kuti kudziwike kuti kumwamba kuli mulungu wamoyo amene sagona komaso saphethira amawona chilichose cha pasi pa thambo. mulungu apitilize kuulula zisisi pa ana ake amen.
@VungaQueen
28 күн бұрын
Amen ❤❤
@wangachindeya8577
28 күн бұрын
Amen
@TamikaKaponya
22 күн бұрын
Amen
@Emmanuelisraelsimbi
28 күн бұрын
Koma ngati mgwirizano watha ndiye tikhale chisankho tu coz utsogoleri wu unasankhidwa pansi pa mgwirizano wa Tonse. Lets vote guys
@RobertNedson
2 күн бұрын
Ambuye apitilize kukudalitsani 🙏🙏🙏🙏musafooke chonde chonde mulungu ali mbali yanu ndi ife ofuna mtendere ndiochitila chifundo malawi aliyese amen!🙏🙏🙏🙏
@AhmadShariff-bk3rr
28 күн бұрын
Mission impossible
@ChifundoNinje
28 күн бұрын
Plz plz achisale amunkhitho plz maso ndinu kt amene mumapeleka chitetezo Kwa Pam
@ephraimphalawala4720
28 күн бұрын
Prayer Malawi
@harrietmkusangombe
28 күн бұрын
God have mercy on our country
@preciouskadembo1932
28 күн бұрын
Dr Bakili Muluzi amkatuza koma ife aMalawi kusamva
@user-tw2zf7bj3e
28 күн бұрын
May Allah almighty protect Apm 🤲 amiina
@AndrewDinala-d9j
28 күн бұрын
Yes
@FrankSpison-o7o
28 күн бұрын
Lord have mercy on us
@wangachindeya8577
28 күн бұрын
Amen
@salimmkumakumakitombi-yc7pw
28 күн бұрын
Uthenga upite kwa Norman chisale .onesetsani kuti chitetedzo chakhwimisidwa pa gate
@user-bd5kw8oq1r
28 күн бұрын
Koma apa pali anthu odwala amene amakhulilupilila social media dziko lathadi basi munthu kungodzuka kupanga plan yoyipitsa munthu basi the opposite is true inu ndi amene mukufuna chakwera ataphedwa mu nthawi ya DPP anthu amaphedwa ambili apa lero iliso layipa bndiyetu sankhani yesu osati satana mudzakondwa
@user-pv9uk6sc3w
28 күн бұрын
End of chakwera and MCP, achepa, wapha uja Chilima wakwana basi. Thanks to Limpopo FM.
@PatrickSomanje
28 күн бұрын
I love u mr khanga osawopa ngwilanani manja pls
@AndrewChilambo
28 күн бұрын
Antanyiwa pitilizani kuchenjeza amalawi zazigawenga za mcp
@tiwongehojaney5873
27 күн бұрын
God will protect Peter ❤❤❤😢😢
@user-pt8wb4vw6r
28 күн бұрын
Inu antanyiwa mwina inuyo ndinu mmapha anthu ndiye mzinamizila ena ndinu zizsilu ndi maboza anuwo
@IbrahimPhiri-ky5jk
28 күн бұрын
Awili aziwika kale tikuimbolani kuti muziwe zosatila anafika pa asoko ndiye atawapo koma tikuwalondolola anyani amenewa komanso mangochi boys ili paliponse 💯
@vituveggah7619
28 күн бұрын
Osazamuphwekesa comrade
@AiwaMedia-sh6vx
28 күн бұрын
Limpopo FM and BAKILI MULUZI TV mukuyesetsa ndithu kutitsegula mmaso koma amene alikutsogolo kwathu n'gokhumudwitsa. A Opposition aliko????
Can I come to Malawi and show my position to chakwera government?
@GrinTemboh
28 күн бұрын
Continue with good news we always listen u ukutimvetsa kukoma ntanyiwa
@ThivadoartistDyson
28 күн бұрын
Akangopha peter l tell you chakwela we come by the trip cross the country kukathana ndi iweyo alu continue.
@user-ky4ce9gb6j
27 күн бұрын
Ndipo kwambiri tu mmm
@kensonmbewe6692
26 күн бұрын
I think this is a sign that we have so many satanists in Malawi, we need God, anthu afika pongoyankhula zimene akugani as long as it will black mail Chakwera, how can you feel if that happens to your father. Too bad
@BlessMnyenyembe
28 күн бұрын
Thanks
@MatemangaMoyo
28 күн бұрын
Limpopo FM ndi bakili muluzi tv, mulungu akupaseni moyo wautali
@loydchisale7077
28 күн бұрын
Mukungobweresa udani apa I have been working there ku page house and no 1 can have access to poison APM the way I know the security there mmm
@vicshyma5644
28 күн бұрын
Chilima uja anafa bwanji . Security analibe
@samuelazumah1050
28 күн бұрын
Chilima kod iwe alikut
@piliranimalama6090
28 күн бұрын
Anthu ndiye kuwadodatu ndi mabodza
@Janaphiri
28 күн бұрын
Munthalika wakuti sangalanulire Dziko la Malawi ali ndi ntchito yanji? Za fodya basi Kodi mwasiya za Tea mwayamba za chamba eti
@user-mi2xf3sw1i
28 күн бұрын
Ku kholo kwa amako wamva
@dalitson3558
28 күн бұрын
Pantumbo pa mayi wako galu iwe
@AREFRIEDNELSON
28 күн бұрын
MCp ndichigawenga kuchokela ma 90s nde wina iziti chakwera Alobwino walowa nzwiwanda wangofika pa misara
@macdonaldkorea2928
28 күн бұрын
Tiyamike kut okonda dziko ngati achina Mtanyiwa alipo ambiri....chifukwa chaichi choipa sichibweredzedwa....a Gadama, Matenje ndiena monga a Chilima ndiena aja akwana, pa Muthalika pokha usayerekedze ndithu iwe Chakwera (kungokhala anthu amagazi basi) Bakili Muluzi amkanenatu kut MCP siyoyanjana nayo lero ndiiyo itangolawa mpandowo basi kupha kwadzuka ASAAAAA
@benjaminjobo3525
28 күн бұрын
Nyimboyi ndaikonda Antanyiwa cain ndi abelo
@adrianobrigida3402
28 күн бұрын
Chigawengacho Chichewa Chakwera chikutseweretsa miyoyo ya wanthu.
@UsenLashid
28 күн бұрын
Mulungu ndiwamphavu yonse Nothing can happen to them in the name of Jesus
@AleksaWilliams-qc6cn
28 күн бұрын
Yoo alipachintchito eti
@JohnFrank-g6e
16 күн бұрын
Ndi Ana awa zomwe akufuna sizitheka komwe in the name of Jesus
@JosephyMakunganya
28 күн бұрын
Nkhope za Rwandans zimadziwika asalowe dara kumeneko
@EliasKawuwa
28 күн бұрын
A Ntanyiwa tengani ndi inuyo dzikoli,musawauze azanu kuti atenge koma inuyo, a Bon Kalindo, wa Bakili Muluzi TV,atenge dzikoli,kuti kunyoza,ndikutukwana kusiye, kumangonyoza basi, zambiri zimene mumanena ndizabodza kwambiri, zonse akunena za Peter Muntharika ndi zabodza zimenezo, kungofuna kudzionetsa kuti achina Peter Muntharika awaone kuti akupanga za iwowo,kuti DPP ikadzawina adzawatole,adzadyetse mimba zawo
Mulungu mumutetezere peter muthalika kulikose komwe apita 🙏🙏🙏
@kangungufoundation2020
27 күн бұрын
Kodi amalawi bingu anakulakwirani chani?? Munamuchotsa mwachipongwe, peter uyu mukuti peter ndimunthu amene munamuchotsa mwa chipongwe again kungoni peter ndi chitsiru akuloranso kuti azapangidwenso chipongwe, saulos chilima zana zanali mumamutukwana limodzi ndi chakwera nde poti lero wamwalira wasanduka wabwino amalawi mulibe nzeru you deserve what is happening and there is no way out until you change, you will reap what you sowing
@user-uk1tt7ho9t
28 күн бұрын
May Lord for everything please protect our beloved president
@OnenessLestas
28 күн бұрын
Zamaboza basi mulungu akuwoneni
@user-ky4ce9gb6j
27 күн бұрын
Best Limpopo fm and BAKILI MULUZI tv MBAMBANDE
@user-ww3fj9oi7j
28 күн бұрын
Guys let's be active, tisapange za Baibulo zonyozera kulowa mchombo
@MuhammadBAKILI-kl2mj
28 күн бұрын
My bsst ladio station limpopo
@patrickkusailemp3769
28 күн бұрын
Longlive APM ..God is in control !!
@user-od6eo5zc4h
28 күн бұрын
Mudzina la yesu christu mnazaleti mutetezelnini Peter mutalika kulikonse komwe kuli iye
@cliftondad3816
26 күн бұрын
Zinazi zalowa fodya zinthu.. apa nde trust pa nkhani zanu ndachosa.... Maboza
@DesmondOzuzu
28 күн бұрын
Komatu one day is one day it LL come back around
@MaureenBanda-t2q
28 күн бұрын
Asiyeni akafa ndiiwowo ili ndi dziko
@christophergibson72
28 күн бұрын
Inu munthu watha kale uyu mufuna mudanitse basi
@JabiluWaiti
27 күн бұрын
Mmmm koma akachoka kwa Peter abwera kwa inu a UDF inunso mukuyenera kukhala osamala
@MarkBanda-w9c
26 күн бұрын
Chakwera u must know hidden things comes on open because of almighty God's power
Пікірлер: 436