On Nyasa VoiceBox, Businessman Mike Chitenje aka Bangwe One refutes claims that he is one of the alleged individuals sent by government to hunt down Owner and Manager of Bakili Muluzi TV.
Ku Nyasa Voicebox, bambo Mike Chitenje aka Bangwe One akutsutsa zoti ndi m'modzi mwa anthu omwe akuganiziridwa kuti anatumidwa ndi boma kukasaka Mwini komanso Manager wa Bakili Muluzi TV.
#malawi
Негізгі бет Palibe Anganditume Ine Kuti Ndikasake Munthu - Mike Chitenje aka Bangwe One
Пікірлер: 66