Chakwera Ambuye amuone ndionse omwe anatengapo mbali
@user-xm3zl5cg6x
Ай бұрын
Yehova amava aliyese apukute misonzi yathu ndi chilungamo
@ruthkundwe7448
Ай бұрын
My president suffered with others on that day,oooh God u r the God who never sleeps, THE WICKED WILL NEVER REST
@user-do2cs8nf4b
Ай бұрын
Zinsinsi ndzayehova, zombvumbuluka ndi za ife ndi ana athu, Mulungu ambvumbulutsa China chilichonse chikhala poyera
@FrynessMoyo-to2du
Ай бұрын
Chakwera unapedzeka bwanji ndi black box asilikari amalawi ndi manyi chakwera nyini yamako 😢😢😢😢
@PreciousBandah-l2r
29 күн бұрын
Mutu sugwela iwe
@cynthiakananji1608
Ай бұрын
Mzimu wa chilima sunagone Uzagona chilungamo chikapezeka. Mukazangophaso a nyamata awiriwa, Mizimu ikupengesani misala baba kuvula kulipo chaka chino
@BlacksonKambazawana
Ай бұрын
Koma chonde chonde izizi ngati zili chotcho sizabwino .komaso azungu awa atiwuze mwachangu mistake its mistake asibisepo munthu chonde timakukondani koma payizi fulumizitsani chonde ngati zinatelo kungo vomekeza mbili siyiphamunthu panalakwika koma zovotela dpp ayi tizavutika amalawi tisakhe chipani china kupatula ziwilizi ngati ndizowona izi koma ngati ndibodza mcp yomweyo.
@alomuddin8801
Ай бұрын
😄😄 CHakwera manyazi bwaaa, amalawi kuwamenyanitsa mitu mmaganinzo Pa ifa ya chilima iwe ukudziwa, apa ndy waonetsa machendeee manyazi bwaaaa
@user-ky4ce9gb6j
Ай бұрын
Ndipo inu esh
@user-yw7qv3ld5k
28 күн бұрын
Mmmhh ayayi imfwa yowawa iyi
@BellaMandala
Ай бұрын
Sitingamangoyasa candle for nothing
@RhulaniMukasi
3 күн бұрын
Anaminyero ose amatumbwa kumapakira chakweraaja arikut Sono nthawi yakwana DC karindo nkhan ndiimeneyo mmawa kofunika kuilengeza zenizen bakiki muluz osaiwara nkhan ndiimeneyo
@rhodahjere8747
25 күн бұрын
Galu kamupeni akapangire kwa make,osati a Malawi ndindaniso angamuvotere
@emilynthite6545
Ай бұрын
Azimangilila ameneyi chikangawai
@isabelmartin7567
Ай бұрын
Mulungu saozela ❤❤❤
@juliusnjerengo2610
Ай бұрын
GPS global positioning system.
@yassinn5634
Ай бұрын
Anamva akuthama ali Geographical mmalo mwa global
@user-bd5kw8oq1r
Ай бұрын
Ayi koma mumatha kitumikila satana inu munakachipeza bwanji kumeneko 😅😅 eeeeeeeee kuli ntchito a Malawi amalawi kodi yesu atakupezani mukunena zopanda umboni mungatani osamvako mu mtima kuti ndikunenazi ndili ndi umboni? 😅😅 manyazi mulibe anthu inu work up time is almost finished Jesus Christ is coming soon get ready before we die
@InnocentEdasi
Ай бұрын
Chilima ause mumtendele
@ChancyJere-pz5sv
Ай бұрын
MCP chomwe yinapanga siyikuchiziwa kom chomwe aziwe misozi yaathu ambiri singapite pachabe muwona mulungu ava kulila kwa malawi
@user-fh7sd6gp3f
Ай бұрын
Shaaaaa kutamba masana mcp😊
@HaliJana
11 күн бұрын
KOMA CHAKWERA NDIWE OLIMBA MTIMA ANTHU 9 UMAGANIZA BWANJI KOMA MIZIMU 9 KUPHA CHAKWERA ULIBE UMUNTHU PANYELA PAKO
Zimenezo nde inu mwazitenga kuti,mu Black box, kapena zabodza zanuzo
@user-ke7ii6ip4s
Ай бұрын
Baliki muluz ali ku tete ntanyiwa ali ku tazaniya
@AndreaLouis-wd8iv
14 күн бұрын
Software which those guys they using l don't even geographic point service it will show 🙄
@user-vu4cz1mt4f
Ай бұрын
Koma mbuz imenei osangoimika manja bwnj coz zonsetu zingofika poyera
@williamsalexmbonga
Ай бұрын
Mzosatheka ukunenazo ase iwe Chimphuno chako
@user-oc9vl9xz8e
Ай бұрын
Zamanyanzi kwambili athawa dziko lokhala lawo
@amoschataika7440
Ай бұрын
Yomweyo Chikangawa 😂😂😂
@christiantattoo779
Ай бұрын
Paline chinsinsi pa dziko la pansi aziona Mulungu amalanga
@Randy-er2xo
3 күн бұрын
Chipulezidenti chakupha
@MariamChipoka
Ай бұрын
Mulungu amapanga njira popanda njira
@chrispahuwa
Ай бұрын
Koma chophera anthu ndi chiyani satana iwe wandiliza
@GriffinDeleleka
Ай бұрын
Masiku ano kuli technology asatengere nthawi ya kamuzu anthu chilungamo amachibisa ndimatha
@Mervic-vm8eo
Ай бұрын
Chakwera pamtumbo pako galu iwe
@MphatsoIshmaeladam
Ай бұрын
Yes that's true ndipo akunena zoona koma afufuza bwanji popanda black box
@WilliamBandaWili
Ай бұрын
Athakati awa koma ndi abusa assemblies fake
@user-xt2gu9yt9q
Ай бұрын
Ose paulendo omwe anatengapo gao koma ziliko
@Malani41
27 күн бұрын
GPS is global positioning satellite! Don’t get it twisted.
@DanielJuwawo
Ай бұрын
Mizimu ndi yambiri zedi kuwapha anthu osalakwa zoona mmmmmmm koma mcp ayi ndithu
@ChiukepochakuzgukaMunthali
26 күн бұрын
Ukuyankhulawe ndi wa MCP. Apa ukufuna kusokoneza kafukufuku wa German. Chonde khala chete tose tiyang'anile chimene a German atanene, mukachulusa zokambakamba choona chenicheni chisokonekela chifukwa oganilizidwawo alibe pa ulamuliro wa ziko lino
Пікірлер: 191