And the people like you is what we need in our country and I'm sure that your work will transform the country, as long as if you have a good support .
@JusticeMaguza-tq2rn
2 ай бұрын
Anayambisa izi ndi Dr Chilima Then kuzamulanda mphamvu tonse mkuthera pomwepo
@itubiz1501
2 ай бұрын
Nkhani sikuti anthu tiwakonde, but we wanted winawake oti aonetsedi kuti zithu zitha kusitha and thats what Mr Usi is doing, sangapange zonse nthawi imodzi but pa size yawo ayamba bwino. He just needs good support but he is capable of changing few things for better way. Even Obama in USA he used to do this kind of strategy or ma prime minister aku England they always do this. God should help you, bless you and protect you mr VP
@williammazizwa1882
2 ай бұрын
You must also visit the Malawi immigration. There's too much corruption there. Especially in Lilongwe a lot needs to be done
@HendricksMkadan
2 ай бұрын
Even Muzuzu also
@giftpeterbanda6274
2 ай бұрын
Blantyre is worse, I paid Mk 400,000 for passport, a passport that is supposed be paid Mk50,000
@sadockbanda1595
2 ай бұрын
Good work bwana VP continue and God bless you, consider visiting Pension and Treasury Departments so many arrears
Anga akupanga sewero ati, komabe thus cute of him...
@JamesChingolopiyo
2 ай бұрын
I appreciate you 😊 Dr Michaels because you have done a good job and that job we will remember you because some people they are negligence
@SaulosMbuna
2 ай бұрын
View his job description..you will agree with me ...vice president yake ndimeneyitu pa job description..adzasinthe kae description yo ...Usi can't operate outside his duty line...he is just following that ..ma vice president ose palibepo chomwe amatithandiza as on their duties
@VioletMkwinda
2 ай бұрын
Ndrama yolipira 2022 mpaka pano za ziii ,Escom sikutithandiza ,keep on mr vp
@BeatriceMitayi-wt3js
2 ай бұрын
Ine mayi anga nyumba yawo 5yrs now akuti mu system ikuwonetsa kuti magetsi ariko eti zowona
@FungulanReuben
2 ай бұрын
APM my vote
@StanleygMagombo
2 ай бұрын
Nice ,it makes people to know what they are employed for. We need to love our Country Malawi. Keep it up.
@YusufSamu
2 ай бұрын
A VP ine ngati munthu am very happy on what you are doing. We have to do our work to serve Malawians.
@danielringo3769
2 ай бұрын
When he visited Chikwawa I heard & read comments by some cilvil servants saying "ameneyu ku office kwathu sangapangeko izi". Slowly slowly the list is getting short. Uyu akupanani m'bomamu 😂😂😂
@MatemangaMoyo
2 ай бұрын
Achosedwa ntchito
@AhmadumkomaTambala-lr9gp
2 ай бұрын
Ngat kuli company yosakonda macustomala awo ndiy ndiescom ngat ulibe ndalama magets njeeee Koma ndalama analandla kale kale tikuvutika amalawi escom yanyanya chinyengo bola water bord
@JimmyMpepula
2 ай бұрын
Appreciate young chief accountant ,you have made me to work hard ,koma usi apitilize
@emmanuelchirwa3420
2 ай бұрын
Well done ✅👍 vice-president ❤❤❤❤❤ good job
@giftpeterbanda6274
2 ай бұрын
We need leaders like Honourable vice president Dr Usi,this is a wake up call for employees who are playing in government departments like kids in creches.Good work Dr Usi for wake up call
@LuciaDyson
2 ай бұрын
Mwina ma certificate akuwolera nyumbawa agwire ntchito😅😅 Sinanga oseweretsa ntchito adzichotsedwa kkkk. Umakwana manganya(bambo a Scono😂❤🎉)
@RonaldPhiri-ib7yb
Күн бұрын
Keep the good work Deputy President Mr Usi
@CatherineBwanali-z1g
2 ай бұрын
I salute you DR Usii... keep it up...i see this wisdom from far in your Tikufelanji comedies
@AnnieBanda-rb2dk
2 ай бұрын
Aaaaaa amalawi akhaulisatu apa asaaaa anasiya kugwira ntchito ulendo kokayinga bwana wapezerera 😂😂😂 samagwira ntchito agalu amenewo amangocheza basi
@PetroKachiwala-hl3hp
2 ай бұрын
This is great VP,we need improvement on how government agencies work. Well done VP
@DickmanMaklaud
2 ай бұрын
Mr VP keep it up. Probe Escom again the protocol they follow to connect customers in districts or towns. They don't follow first come, first serve. Check account komwe kumalowa ndalama za Escom customer akalipila, then check which customer is connected first e.g at district level, then you will understand Escom is not fair
@kamenakedrick7644
2 ай бұрын
I love the way is handling things in Malawi usi keep it up boss
@StoneckJali
2 ай бұрын
Amalawii jelasi malo moyamikira mukuganiza za alawasi .Usi go ahead
@LazaloZimbili
2 ай бұрын
Kkkkkkkkk kabe naye akufuna ka period kasalaka akhale ngat
@PriscillahLombola
2 ай бұрын
Ndipo akuenela kumpasa kumene,amafuna adziendela ndalama zake eeh,amalawi unakula ndi ufiti.
@PatrickIsaac-m1z
2 ай бұрын
Usi, you're doing the best
@InnocentJames-q7o
10 күн бұрын
Keep it up Mr Vp we need people like u
@RichardChavula
2 ай бұрын
if this can continue Mr VP I believe things can change in our country. keep it up
@yohanethom2164
2 ай бұрын
That's a leadership experience we want in our country I like it boss
@MarvinPeason
2 ай бұрын
I like the move that's the same move late SKC started with but later anatsamitsidwa may this continue n bring a positive impact to the national
@innocentmayenda
2 ай бұрын
Nice advice to both escom and the young accountant.
@festonMatiki
2 ай бұрын
Michael your doing a very good job kip it you inspire me
@WilliamMtachi
2 ай бұрын
Big up Aurlings, you handled the VP with professionalism
@emanuelphupha19
2 ай бұрын
Amazing and excellent work Mr Usi. This is what will lift up Malawi
@MeikleReuben-l4x
2 ай бұрын
This is a man what Malawians need
@HastingsKadzanja-c4y
2 ай бұрын
USI keep it up wandikumbutsa chilima
@JonathanLimunye
2 ай бұрын
We Malawian we want you Mr VP to proceed these in all sectors wina asakuchenjenekeni we are following and we are here to see transparency and accountability
@AfricanKingdom-uv1qb
2 ай бұрын
I appreciate you Dr usi keep it up
@kensonmbewe6692
2 ай бұрын
This is beautiful, civil service must change, ku MRA nso Mukawoneko
@EmmanuelMalunga-o7k
26 күн бұрын
Miyambi ija ndyofunikad "don't judge a book by its cover" l salute you bwana VP🙏🙏
@victorbanda2468
2 ай бұрын
Ministers should be doing this, surely we can improve as a government 🎉
@PriscillahLombola
2 ай бұрын
Aba nthaw zanji?😂
@GamaGama-z8p
2 ай бұрын
Michael usi he need to be given the political award of the year
@WasiJala
2 ай бұрын
I like the way vp is doing keep up mr vp
@ChipiliroLungu
2 ай бұрын
Ndapezapo vuto kwa ogwila ntchito yo akuwopa pena pake inu mujuwona bwanji? Good work Mr vp
@zioneabuali
2 ай бұрын
Mubwereso Ku Lilongwe Kunoso bwana
@EsnartMartin
2 ай бұрын
Ndayamba kumumvetsa vp and okhawo odana ndi dziko lawo ndi omwe azifinyika keep it up
@chifunirosambakunsi6860
Ай бұрын
Impressive a VP that's what we need kuti ogwira ntchito azikhala serious ndi post yawo
@ChimwemweMuhelliwah
2 ай бұрын
Good move a VP...muptenso ku judiciary uko kuli zibwana.. milandu kumatha ten years sinalowe mkhothi...
@jameschakholoma8461
2 ай бұрын
Wandisangalasa kwambiri vice president Michael usi ngati SI manganyansotu nkhani yabo keep it up in all public sectors
@JACKREENEBANDA
Ай бұрын
Good work bwana vp your big than mulanje mountain
@KimJime-d9k
2 ай бұрын
Good work our vice president kumeneko nde kuchangamuka Apa nde mwaigwira ntchito
@masakaunga4099
2 ай бұрын
Wow amadya ndalama mosatulutsa thukuta mma ofesi mu continue Utsi
@SandrrahAmin
24 күн бұрын
Mr vice president i really appreciate it 🙏🙏 good work
@LindaSonipa
2 ай бұрын
Good job Mr VP,,,,,, Amalawi tikufuna mtsogoleri ngt inuo 🔥🔥🔥🔥🔥
@RodgersPhiri-b3r
Ай бұрын
This kind of leadership it's what we need in our country
@KasimbaMwandira
2 ай бұрын
Very good.. That's the only way to renew our services
@alexanderlipenga1330
2 ай бұрын
This is what happens in public offices ma controlling officers sakhala mu office kuthamangira ma meetings for allowances kusiya ma junior akutipula, they don't delegate. Koma za udzuu they delegate
@noelkaunda
2 ай бұрын
You have a great 👌 😂 Job sir thank you 💕
@EricBotha-g4t
2 ай бұрын
This is first time for me to see VP go checking every corner of our country... Please bwana go ahead maybe we can survive Too much corruption as well
@DarlingtonChaura
2 ай бұрын
Bravo ine ndinalipira magetsi ku escom 2021 May. Mpaka lero August 2024. Sanalumikize.
@HamanjaManyela
2 ай бұрын
DR VP please come to Lilongwe
@symonTchale-dg3on
2 ай бұрын
I like what he is doing, well done.
@jomochirwa
2 ай бұрын
Mumazolowela ku malawi inu amene mukugwila ntchito mma office simulemekeza anthu wofuna kuthandizidwa akafika pa office pano mumatenga tchito za boma ngati zanu.
@AllanKadzako
2 ай бұрын
Recommendable job please God Bless you Sir
@RenfordLevison
2 ай бұрын
Good work Mr. Vp zikanatero bwezi Malawi alibwino.
Big up to the ESCOM Chief Accountant, that guy is a professional, 101%
@chikondichakwana168
2 ай бұрын
I like the advise part "your Seniors are retiring soon but you are still here, so don't spoil your carrier"
@ALEXANDERMDOKAM-rq8tw
Ай бұрын
Keep on schooling them we want a better malawi for all.Ulemu wanu a VP.Keep the fire burning.All the best.Ku MRA mukawaphunzitsenso kuli ena amaitenga MRA ngati person entity.Koma a Bizwick amatchinga kuti uwonane nawo popeza amadziwa kuti zomwe iwo amachita mma office a mmusi ndi zachinyengo komanso zolakwika.Ena akugwira ntchito modzipeleka komanso mwadongosolo.Komanso kuli ena kumeneko ndi mma department ena a boma omwe akuzuza anthu.Keep on schooling them
I like this ineye mages kulipila 2020 February till today only stories I regret being a Malawian
@KuntindiDali
2 ай бұрын
Zipitilire. Tikanakhala izi zidayamba kare, mbwenzi tiri pena pake. Ayenderenso mmalo ena omwe anthu amalembedwa ntchito. Ena amalipiritsa akafuna kulemba anthu ntchito. More fire Mr president vp. Andrew nyimbiri
@DianaSuluma
Ай бұрын
Nice job
@BaxterKachelenga-mb7wx
2 ай бұрын
I am proud of these visits for a long time goverment services mumachitika zozunza anthu oyenera kuthandizidwa,pomwe boma NDI lakhala likuphunzisa mmene anthu angamagwilire ntchito Koma why makapani wamba amakhala amachawi kuposa a boma?And anthu nkumavutika kuti athandizidwe.Mr vice president pitilizani komanso Kwa olamula osatirawo should continue this .
@MzikaPhiri
2 ай бұрын
Kkkkkkkkkkkk koma VP ayi zikom mukutimvesa sugar keep it up....
@maya6609
2 ай бұрын
I don't know if what the VP is doing is right or wrong but it's a lesson to all of us working in offices whether in Govt or private sector. We need to be on our A-game everyday for the sake of the people we serve, the companies/organizations as well as to avoid embarrassment.
A chilima anja adali wokula mtima sorry sibwino kunena munthu wakufa koma adali ndi maganizo achabe
@DemobryKautsi
2 ай бұрын
😊@@HendryChiwezo
@mphokadyson4158
2 ай бұрын
Siyofunikanso kuilemba just come back to this video bas kkk,, but am impressed with the chief account has confidence
@EdessChozex
2 ай бұрын
If all V.P was working like this one bwezi titawona kusintha mmalawi long live mr Usi
@BlessingsMakalani
2 ай бұрын
💯🙏🙏ife before it was like this Malawi it was good country
@MichaelWilliamsNyirenda
2 ай бұрын
Exactly 💯💯💯
@TamandaChimwala
2 ай бұрын
" First come first serve" .. a rule of big thumb has to be applied in all public sector for the development of this country . Vice P Michael Usi ..Bwana tiyamikile pa ntchito mwayiyambayi musasiye muyendeso ku ma Department enawa.
@nkosikhonasiphiwemdlalose227
2 ай бұрын
Leadership from the heart and anointed
@RashidKazawe
2 ай бұрын
Ngat ndkuonera move😁
@jonathanmaseko6057
2 ай бұрын
This is good work
@ThomsonNyirenda-df9io
2 ай бұрын
Keep it up vp the good work try to change malawi please💪
@GeoffreyMguwera
2 ай бұрын
This's the kind of leadership we really want.
@TsogoloCommunity
2 ай бұрын
Nyc work Mr Vice P🎉
@dumisaniphiri3687
2 ай бұрын
eeeeh kungolowatu amvekere odi! atalowa kale kkkkkkkk koma this gent amandiwaza 😆😆😆😆😆😆😆😆😆😃😀 henewe good job
@FrancisKalimba
2 ай бұрын
Mr vice president good work,,,,,God blessed Malawi 🙏🇲🇼🥂
@theologybakali2738
22 күн бұрын
Good work boss
@FareedahLapken
Ай бұрын
Bravo Mr VP...I salute you
@RazzaaqSandali
2 ай бұрын
Fantastic, well done Mr president
@AubreyNdeule
2 ай бұрын
Keep it up Mr vp
@Glorynkhoma-m2y
2 ай бұрын
Mukanawafinyanso mbali ya ma laity anthuwa akupanga zobowa awa ndipo saopa Mulungu awa amazunza kwambiri anthu ena analipira kale mpaka pano poti alibe say, thanks bwana USI keep it up mupitenso Ku water board
@emmammatsa1284
2 ай бұрын
Thank you Mr VP president, i wish if you visit all other organisations including waterboard please, too much corruption
@kantayeniphiri4016
2 ай бұрын
Good work bwenzi tili patali... Viva government
@KimJime-d9k
2 ай бұрын
Kwambiri tu anthu awawa adakati anali angapo bwenzi tili patali
@uchizicmakala
2 ай бұрын
This is not political issue but visiting the office ndewina kula nkhula kut si skc ayi please OK ukhale iwe chabwino kkkk keep it up Mr vp
@BlessingsMakalani
2 ай бұрын
I like what you doing Mr Usi problem is that way you take from MCp
@emmammatsa1284
2 ай бұрын
I applied my electricity 1 year ago, sanabweretsebe, i am considering solar panels now
@ngwilasephron7197
2 ай бұрын
Escom di anthu corruption so much they can get money from you and nothing good for you .
@Eric-gb9ms
2 ай бұрын
My question is why Mr chilima the didn't give him this job he was always in court
Пікірлер: 610