Nkhani ikhale UTM , AFORD ndi UDF apange alliance, president achoke ku UTM ndekuti azapeza ma vote Ku north , central pang'ono koma ochuluka ku southern nde kuti azaiphula bho bho
@AnthonyPhiri-qp8fn
26 күн бұрын
Mr bon kalindo thanks live on zambia Lusaka
@KhalideNerve-mu1eq
26 күн бұрын
Mission possible
@user-iz3qr1gu9d
26 күн бұрын
UTM welcome back to DPP family
@mishasjambo4793
26 күн бұрын
Eeeh ndine bon ...... 😂😂😂 Kuipatsatu fireee
@Yuze_Matukula
26 күн бұрын
Boooooooooon Kalindo!🔥
@OmecxKondwan-dx7do
26 күн бұрын
Mr DC hohoho🔥🔥🔥
@user-wh6zp4vx1n
26 күн бұрын
Chikati hahahaaa Ndipo chimaseka modelela Chi Born Kalindooooo
@chrisneySwanepoel-yu5vd
26 күн бұрын
Born kalindo ndakamuna
@IssahAluba
26 күн бұрын
So good 👍
@McDonaldMakina
26 күн бұрын
Pangolini tsopano
@daudinussah2232
26 күн бұрын
Ubwino wake ovota ndife, and kalikonse kochitika pansi pathambo Mulungu amachionetsa poyera
@GogoKasiketi
25 күн бұрын
God first
@PemphoSmart
24 күн бұрын
Propaganda at its peak. Ife anthu osauka takana kuti ndiwe president wathu
@InnocentSayenda
25 күн бұрын
Mmakwanila big
@GeorgePhiri-ub2of
25 күн бұрын
Pakhala mabvuto olimbilana utsogoleli APA ifee phee Ku MCP basi
@AlbertNambwale-sm9qe
25 күн бұрын
Well did L
@user-wi9pe2hz7e
25 күн бұрын
Mawu a Bon sapita pachabe nd Yosef mwana wa maloto😅
@desmondshugar4585
26 күн бұрын
Good
@PeterJanga-wv9nz
25 күн бұрын
Born kalindo akamuna bambo
@Africanbwoy185
25 күн бұрын
Uthenga ukupita kwa Michael Usi aka Manganya
@AlidiMdala
26 күн бұрын
Munyengo yong'alula🔥
@RuthChilobwe
26 күн бұрын
UTM ISAPHATIKIZANE NDI DPP CHIFUKWA MKAZI WA LOTI ANAYANG'ANA MBUYO POTHAWA MOTO KU SODOMU..PAMENE NGELO WA AMBUYE ANAWAUZA KUTI ALIYENSE ASAYANG'ANE MBUYO. KOMA MKAZI WAKE WA LOTI ANAYANG'ANA MBUYO POGANIZIRA MOWA WAKE WOMWE ANKAPHIKA KUSOMUKO NKUMAGULITSA. IYEO ANASANDUKA CHULU CHA MCHERE. SO UTM NSO MUKAPHATIKANA NDI DPP MUSANDUKA CHULU CHA MCHERE.MUKHALA STUCK AND DORMANT DEAD WOOD .!!!
@EdisonNgolomibanda
26 күн бұрын
Carry on pangolin
@SteveGemini
26 күн бұрын
This is boooooooorn Kalindo🤣🤣🤣💯🔥
@ChifundoNinje
26 күн бұрын
This is the truth utm plz bwererani ku dpp
@raymondlupiya
26 күн бұрын
Ichichi chinabwera🔥🔥🔥.
@Yungjoe786
25 күн бұрын
Pangolin iweyo the DC
@LDeeNdilimunjila-zs1qh
26 күн бұрын
Born!!!!!!!!!!!! Kalindo!!!!!!
@heavenpromotions
26 күн бұрын
Akuti anzanu wo anavota kale😂😂
@YusufujohnSeruweke
25 күн бұрын
Chilungamo kalindo
@RuthChilobwe
26 күн бұрын
And madam Patrucia Kaluati being the leader of utm presidential.candidate.cos she is has got experience of leadership.by profession she is a teacher and again she has experience of political leadership.she was in dpp .wurh Bingu wamutharika and peter mutharika
@user-xn5jl3sp6d
26 күн бұрын
Born💥💥💥
@MarkTembo-ut9sv
26 күн бұрын
Ku dpp tikataniko? Chilima anatulukako ndipo sanabwelere mpaka kufa kwake ndiye ife tufuna mufuna mzimu wake utikanthe?
@MosesNjanje
26 күн бұрын
Ndeee kupusako do you think kut utm payokha ingagwetse mcp yotiiii ili m'boma inuyo dziko lanu simulikondayiiii amkolo chilima ananena yekha kut ku dpp anachokako analibe vuto lililonseee ndee inu ndare simuzidziwa Bola mungokharah chete ngt muganiza kut mungazawine panokha kuchotsa chipan cholamulachi
@franciskameko2586
26 күн бұрын
A UTM panokhs simungalamule dziko ndpo position yanu izingokhala 3 or 4... Koma chifukwa chot ndinu okulamtima mumadzimva ngat muli nkuthekera... Kachipani ka ma MP 4 koma matama thooo🤣🤣🤣
Musiyeni Manganya asangalale ndi mdalitso wake, ndi Mulungu adalola kuti akhale pa mpando umenewo. Sizoti iyayi wa UTM weniweni apange resign, kuti chani? Kulephera kwanu musade nako anzanu amwayi.
@inessmsiyambiri8517
25 күн бұрын
Hehehehehe kweeee ulira sunati
@MEDSONMZUMARA
26 күн бұрын
zoona kalindo chilungamo
@user-de9nx7ts2d
26 күн бұрын
kung'alura
@isaacpiyo6792
26 күн бұрын
We are not going for coalition again
@franciskameko2586
26 күн бұрын
UTM chipani cha pa social media🤣
@christopherpetro-pen3678
26 күн бұрын
Komatu ndiye kuli kung'alula🤦
@chisomogareta1958
26 күн бұрын
Uyusotu amangolubwa
@richardkuwani3647
26 күн бұрын
Chayankhula bwinotu
@HarryKumwenda-jm1df
26 күн бұрын
Utm
@SwazzyCassium-u9n
25 күн бұрын
😂😂😂
@itzfazmuslimah
26 күн бұрын
Uyuyu ndi 🔥🔥🔥
@RuthChilobwe
26 күн бұрын
Correction utm has vast followers so let utm.stand alone..and its gonna win with the majority.nos
@EvyEvy-my9mj
26 күн бұрын
😂😂😂😂
@gideonnyasa
25 күн бұрын
A Kalindo zindikirani ichi dziko la Malawi ndi latonse, is not about resignation of its members in government positions. Stop misleading people, eg Usi won't resign cos he is serving Malawians not MCP.
Пікірлер: 116