Umenewu ndiye utsogoleri munthu wa Mulungu asamaope kuyankhula chilungamo , osati azibusa enawa kungowapatsa ndalama basi kusekelera zopusa , ana anjoka Inu Mulungu akulangani
@user-pv9uk6sc3w
26 күн бұрын
A Bishop mwalitha bomali, ndipo kumene ali Chakwera sakugona ndi m'mene mwatulukila ma Bishop. Chakwera ndi boma lake la MCP lalephera tatopanalo.
@MeckMdoma
22 күн бұрын
Dpp nayo tinatopa nayo nkuona tinayithamangitsa. Mavuto ali mdziko muno solution si dpp. Awa adzawonjezera kusawuka kwa a Malawi kupsola apa. Malawi is going througheconomic problems because dpp mismanaged this country's economy.
Amen and amen inenso ndipemphelo langa ambuye afute ma vote abale anga zoona zomwe timaziyembekezela sizimenezi ayi
@JustinChinombo-dy6tp
23 күн бұрын
Amen amen a bishop mulungu wathu salephera, Achilima anati mudima or ukule bwanji koma kuzacha ndithu ❤❤
@user-oc9vl9xz8e
26 күн бұрын
Azisogoleli ameneqa onse alandile ma thembelelo kuyambila ana awo komanso zizukulu zawo za ana awo onse amene azadye ndalama zomwe akubasi za anath osauka alandile thembelelo ndibkhate mu zina la yesu....
Father mupitilize kumuthira fire chakwera,watikwana
@CharlesChagudubuka-rm6bh
23 күн бұрын
Akuti apule chasanduka choseketsa 😂😂😂for
@MestreMaday-fv7qo
18 күн бұрын
Chipan ali nacho ndi mulungu wathu
@ThokohPrescotKalonga
26 күн бұрын
Zowona ndithu, malawi akufunika ma demo kuti akozeke
@WisikiBlack-gj4gu
26 күн бұрын
Ameen ameen abusa. Apa boma palibe koma chizuzo basi kuononga dziko uku. Koma apa pakufunika nkhondo ambuye atithandize.chifukwa ngati afika pomupha chilima ife ationa ngati ndani.koma nkhondo ndimeneyatsala basi
Mkwiyowutu ukuchedwa. Ine nde ndikuufuna nsanga nsaname
@doreenkaliati3166
25 күн бұрын
Ulemu wanu Abusa ❤❤❤❤❤❤
@ChilangoNdalama
25 күн бұрын
Amen abshop
@isabelmartin7567
19 күн бұрын
Analowa mu Zina la ubusa 😢😢😢osaziwa satana watola joker eeeeee ai chakwela wapweteka Malawian 😭😭
@PeterChuma-yf1ps
18 күн бұрын
Vote yanga naneso itengedwe
@user-do2cs8nf4b
26 күн бұрын
God is speaking to the government of Malawi anayiwala kuti kunja kuno kuli Mulungu, akupembedza ndalama. Mulungu dzukani pa mpando wanu wachifumu mutimenyere nkhondoyi
@user-vm7iz6oz6r
23 күн бұрын
Pano agula mifut malo mogula makhwala zipatalam
@user-uf4db7im7d
9 күн бұрын
Mwaputa a katolika ndipo simunati muziona, campaign ali mmatchalichi
@HassanJameskananjie
23 күн бұрын
Kod amalaw mupepela mpaka liti lawyer nde kuti chan
@sthoramexjrsa902
26 күн бұрын
Amen father 🙌🙌🙌
@munashemoyo4190
26 күн бұрын
Amen father Amen mau mau
@JamayakoJamayako-rv2he
18 күн бұрын
Mateyu 18 vs 18 Yomweyoo ikhake nyimbo ndi chitsogodzo kwa ife
@MarthaMbewe-uk5nn
23 күн бұрын
Pharaoh watsala pang'ono kuonetsedwa ukulu wa Mulumgu pompano aziona iyeyo kodi sakuona kuti ulemu wake unachoka Kale kale? President wanji omangotukwanidwa mgati chitsiru?
@RachealHarawa-xc9gs
25 күн бұрын
Chilichonse chili ndinthawi koma na apapa zafikapa Ambuye chitaponi kanthu mwasanga
@PaxKinley
20 күн бұрын
Ndatenganso nane VOTE yanga
@gracekamzati
23 күн бұрын
Ameni abusa ine nde sinavotereko ndipoyamba pomwe ili siboma ayi koma kupha anthu
@MarthaMbewe-uk5nn
23 күн бұрын
Tathokoza abusa ameneyu musasiye kumudzudzula pali mau amanena kuti :ONDIUZA ANALIPO KOMA KUSAMVELA KWANGA KWANDIPWETEKETSA
Wakutumani ndimulungu lankhulan mosaopa chifukwa malawi waonongeka ndi chakwela
@user-fe7fb3nw5h
26 күн бұрын
Emen ambuye achitepo kathu ndithu
@BlessingsMakalani
26 күн бұрын
Amen Amen
@gladysbonongwe1038
26 күн бұрын
Amen
@IsaacMusa-py2jm
26 күн бұрын
Mau amphanvu 🙏
@user-uy8uk7so9d
7 күн бұрын
Munavotela zisilu kodi nanu
@user-uc1pd1tc2x
26 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂Koma guys ine ubwino wake sindinavoterepo chipani chilichonse than DPP chibadwireni😂😂 Thalika eeeeee ai ndithu ubwino wake amakamba chilungamo 😂😂😂😂😂😂
@MalawianCamera
26 күн бұрын
@@user-uc1pd1tc2x 🤣🤣😂 akhale ndima lawyer 20 tu uyu
Пікірлер: 171