That's very wonderful massage it's true,tiyeni Malawi tisegule maso
@EmmanuelThambo
3 ай бұрын
Umboni tauwona kuno ku Zomba ma centre ena anatsegulidwa kwa 5 days ajambula kwa masiku awiri masiku enawo amati mafuta anawathera mu magenarators. Keep it up Kalindo we're proud of you.
@AmirGeloo
3 ай бұрын
Why translating it English ?
@JoshuaMagodi
3 ай бұрын
Umakwana ase
@FridayMpanga
3 ай бұрын
❤
@NASP-g7h
3 ай бұрын
Kom mcp kuwina tizavotaso cz axakhala kuti abela 99
@charlesmuwanya7845
3 ай бұрын
Please a Law Society of Malawi ndi zipani za opposition zonse pitani Ku court mukane mfundo yoti opanda National Id asavote. Kuchokera pachiyambi timavota polembetsa mu voter register pogwilitsa ntchito passport, driver's licence,Kalata yochokera kwa mfumu etc . Every Malawian above the age of 18 is eligible to vote without National ID restrictions.
@ZionekaMember
3 ай бұрын
Mwana oopsa kwambiri the DC
@limbanimtitima9170
3 ай бұрын
Awa ndi big man amayankhura chilungamo ❤
@AlexPhaloni
3 ай бұрын
Muthu openga ndiyekhayo angasapote mcp
@JosephMichael-x7v
3 ай бұрын
I wish bon kalindo atakhala president ku Malawi
@BhekiMavundla-po2bq
3 ай бұрын
Zonwe akunena Bon Kalindo zokhuza NRB ndivomelezane naye ndithu,kuno Kumangochi zachitika ndipo zikuchitikabe madela ena.Pano anthu ambiri asiyidwa mu masenta olembesela zaunzika kut alephele kukhala ndichipatso chaunzika ndicholinga kut anthu asazavote ambiri kuno kumwela ndipo Ineyo ndimboni ndithu kwa Born Kalindo.Pa anthu okwana 300 pamudzi uliwonse amene alembedwa zaunzika ndi anthu okwana 100 akha basi Kumangochi kuno,ambiri enafe tasiyidwa akuti nthawi yatha sapitiliza koma 2days yokha ndimene akhala akupanga process ya NRB mumasenta onse kumangochi kuno
@amosphakira7936
3 ай бұрын
Mr kalindo ,mfundo imeneo ndiyoona a kufuna kubela ma vote njira yake imeneo .Ndie ndikofunika kti anthu asavotere through l D chifukwa xisokonexa xithuxi pls.
@MiddayDeleza
3 ай бұрын
Ndalama ndi zimenezo koma mzipatala mulibemo mankhwala shame. Bon kalindo Mulungu anasankha inuyo ngati ngelo wamulungu pakati pa dziko amalawi I silute you
Wanthu azavota ngakhale alibe cha u nzika ngati bungwe lo imirira chisánkho achite zopusa Litha, Chakwera wapha Chilima.aliyense waziwa Ndipo Chakwera pa nyero pa mache
@davedavie6211
3 ай бұрын
Ukhalise DC Ukutisegula maso
@YamieManda
3 ай бұрын
Muthu uyu wa dpp,osangobwerela ku dpp bwanji mbuzi yamuthu iwe😊
@RoseMkandawire-e2g
3 ай бұрын
😂😂😂😂 a president ndeno mukuzikanda pasaya apo pakuyabwa mumanivesa kukoma inu aboni pangani chipani tizakuvotereni ife anthu osauka chonde
@ELINATengule
3 ай бұрын
Akalindo mulungu azikutsogolerani thawi zose❤
@Centre-m6f
3 ай бұрын
UTM ingotuluka mwachangu isanafike thawi ya campaign
@williamdaka79
3 ай бұрын
Anzathu ku Kenya amuonetsa Ruto koma ifeyo a malawi Kaye tinabadwa bwanji?
Zoona zake DC umakwanira iweyo tikavota bas ooanda cha uzika
@LawrenceDickens-jk3zx
3 ай бұрын
End of MCP ndanena ndanena /wetting zachitika ku Kenya basi!!!!
@EliasOdala
3 ай бұрын
DCcc ndiwe katundu omanga ndi wire always proud of yu
@JackMvura-ik2td
3 ай бұрын
If only your family will vote you can talk that rubbish MCP it's not the way simple you think most MCP members they don't respond rubbish the don't talk nonsense they make sure keep quiet no fight with empty teen wait and see chakwera is not a small boy of Malawi so he is always showing the nation of Malawi that he is full grown up man always is away from the stupid people 2025 be careful
@UTHMAN-WAYA
3 ай бұрын
@@JackMvura-ik2td🤣🤣🤣Inu MCP ikumanga anthu ndemuzit ili Quit aaa🤣🤣💔
@LawrenceDickens-jk3zx
3 ай бұрын
@@JackMvura-ik2td uziwo ase kapena umadyanawo za chipanizo? Zako zimene asaah.....
@JackMvura-ik2td
3 ай бұрын
@@UTHMAN-WAYA police kapena MCP tell people the truth don't just talk cause you can talk what I need people must go to court tell them MCP is no longer MCP is a police but talking while you're sleeping by house it won't solve the problem
@JosephMichael-x7v
3 ай бұрын
I wish bon kalindo atakhala president ku Malawi
@JosephMichael-x7v
3 ай бұрын
I wish bon kalindo atakhala president ku Malawi
@PeterRabson-z3w
3 ай бұрын
Ndipo ñdinu nokha otimenyera ufulu
@AndrewWyson
3 ай бұрын
Pompano 😅Kenya Kenya game ndizikwanje
@JamesTobiasNkhoma
3 ай бұрын
Thanks kalindo for the good information.....keep it up am behind u
@IsakyIsak
3 ай бұрын
Chakwela awukhudzidwa za ifa ya saulo chilima
@samdiverson9733
3 ай бұрын
Tivote ndi ngati kale ma id tilibe
@CatherineDesire
3 ай бұрын
🔥New clear BOM,Bonn Kalindo!
@ShiraKasekaNyirenda
3 ай бұрын
Timadalira inu bwana DC mumatiyimila amphawi
@FrankChingudu-pi8kn
3 ай бұрын
Muleken mwana wa eni alankhule za kumtima kwake.
@MeniyaMikaya
3 ай бұрын
Openga kwambili ndiyemwe angabweleleso ku DPP mutu wake unayima fwetseke zanu ndi kalindo wanu yemweyo mwalandila ndalama kwa gogo wanu opanda mano mkamwayo ndinu zitsilu shupt
@MbaulaJames
3 ай бұрын
Lemekeza atateako ndi amako kut masiku amoyo wako apitilile
@AdamChirwa-u3d
3 ай бұрын
Ulem wanu mnthu wamkulu kwambili
@AdamChirwa-u3d
3 ай бұрын
Ulem wanu mnthu wamkulu kwambili
@EliasPhiri-yv8gv
3 ай бұрын
Koma uyu Nde amatokotadi eish
@peterchikwakwa8476
3 ай бұрын
For sure this is State Capture
@HamzaMkwanda-bh8dc
3 ай бұрын
Chakwera why are you evil 😈 Chakwera why are you wicked God will punish you soon
@MussaHassani-zg1hm
3 ай бұрын
Is our president thanks
@RodgersChikumbutso-jr7fh
3 ай бұрын
Ichi chimandisangalatsa
@Jasper-xk9iv
3 ай бұрын
Tili pambuyo pano DC
@WilfredYekha
3 ай бұрын
Mbambande, keep it up
@JamesPonds-j9v
3 ай бұрын
Big up our own DC
@JohnJohn-og8rt
3 ай бұрын
Zoona big man kalindo
@MercyChavula-qy1my
3 ай бұрын
Mumakwana ulem wanu
@NumeliKambo
3 ай бұрын
Born kalindo nd Dolo
@MacKamanga
3 ай бұрын
Wake up call
@MarkKaliati
3 ай бұрын
It's fact
@MessiahPitros
3 ай бұрын
It's true
@KelvinBAligiza
3 ай бұрын
Bg up Dc
@Mpondapromise9
3 ай бұрын
Big up DC
@EsetaGerate
3 ай бұрын
DC 🥰
@SenzoKatopola
3 ай бұрын
Umakwana fadah
@Djmsakama-kj3ne
3 ай бұрын
Osamabisila
@YammsyZebron
3 ай бұрын
DC ❤
@EviePhiri
3 ай бұрын
Dc
@FanizoKawindula
3 ай бұрын
Chitsiru ichi
@SelinadeniasDenias
3 ай бұрын
Ulemu wanu
@MacleanKwacha
3 ай бұрын
Ulemu wanu big man,mumatiyimilila
@frankjolijo
3 ай бұрын
.... Kuswa kuswa....opha mnzake, naye aphedwe
@MasterHeadson
3 ай бұрын
📌
@AkibuMdala-sr1dy
3 ай бұрын
❤❤❤
@MauriceTayali
3 ай бұрын
Ndalama za satanic, samalani. AMALAWI amzanga dziko ili laipa satanic yalowa mudziko lathu ili CHAKWERA atipereka kwa satana
@RhulaniMukasi
3 ай бұрын
Pari galu wina mmenemu waremba masege yonyoza chilungamo cha DC mancgendeake ameneyo mot Malawi mmene akuvutikila ndipo ndikuuzen agalunonse zomwemwaba mukudyazo mukanyera mundende apa sitikusekerelan tatopananu iwenamachende chakwera segula zimakhutuzo uve nthawiyanu yatha
@HarlodLemwe
3 ай бұрын
kod bwana DC ukamapanga zimenezi umafuna chani kwenikweni ??? anthu andale awa amafuna kumatisokoneza anthu akumidzife mbolatu iyi
@LeviChakwira
3 ай бұрын
Campaign will be easier for opposition parties. A mcp apha chilima. 90% ya anthu mu Malawi akuziwa kuti mcp ndi amene apha chilima.
@StevenNathaya
3 ай бұрын
Bwana Dc mumakwanila hvy ndipo musasye kutimenyel ufulu
@chitanibenito1109
3 ай бұрын
Izi ndizoonadi ku south kuno nrb palibe chikuchitika ife tikudabwa kuti a oppositions Ali kuti??? Nkhani ya ziphatso ikuyenda bwino only central region wat is this after all?? Nrb ikufunika kuyipangira ma demo akuzolowera tsopano kaya adya ndalama azisanza ndithu.
@johnchitenji4
3 ай бұрын
Big up born kalindo With powerful message 👍
@ThivadoartistDyson
3 ай бұрын
Chilombo chachilungamo koma bon kalindo mulungu akutetezele until nkhwandwe itachoka 'l think akufuna tipange ngat anthu akukenya.
@LeviChakwira
3 ай бұрын
Palibe munthu amene angavotere nkhope ya chakwera ndi mcp. Never
@sukiemapemba4094
3 ай бұрын
Tizavota zopanda ma ID apo ayi miyala izagwila ntchito kuphanakuphana basi
@VioletMovella
3 ай бұрын
Born kalindo umatiyimilila,,,tili kumbali yako Malawi cwa mun2 uyu
@GetrudeBanda-sd1yf
3 ай бұрын
Osafooka go on
@WinerdShadreck
3 ай бұрын
Aliyese akavota
@juntoiman
3 ай бұрын
Mr DC timakunyadilani Cox mumatisegula maso and mumaima pachilungamo
@MartinKapanga-q6m
3 ай бұрын
ndimakukondani a born kalindo ❤❤❤
@GanizaniPhiri-f2i
3 ай бұрын
Umakwana mr DC tingopita pa nseu basi .mbuzi zimene zatitopesa kwambiri.
@MeliaMichael
3 ай бұрын
I support the motion Pamene anthu akuvota NRB izakhare pomwepo
@ChimwemweKondowe-nj4lx
3 ай бұрын
Ayaluka akubawo
@AbdikaniDasar
3 ай бұрын
That's powerful message continue to show them the right way to catch this big fish mr nyo
Пікірлер: 195