Powerful message,,,we silute you,,,, keep on doing this please
@PrinceBlessings-bv5bs
2 ай бұрын
I hope bishop mwatumidwa ndi mulungu ❤❤❤❤
@HevenChiwaya
2 ай бұрын
Mathembelelo akhale pamutu pa onse amene anakhudzidwa ndi imfa ya a Chilima ndi anthu 9 mwadzi wawo ukhesedwe pamitu pawo omwe anapanga izi Mudzina la Jehovah's...Amen..
@EdenEreneo
2 ай бұрын
Tsoka kwaiye anatengako mbali pa ifa imeneyi sazaona mdalitso Amen 🙏
@BlessingsMassi
2 ай бұрын
Amen
@MathewKalinkhu
2 ай бұрын
Mmmmmmm, koma a Bishop inu mwamaliza zonse, ndipo kumene aliko mutu waima Chakwera ndi boma lake la MCP. Tili pa mbuyo panu Bishop, osafowoka, osatopa .❤❤❤❤
@Ybm-o5y
2 ай бұрын
I will vote next year because of chikangawa accident witnessed by my naked eyes,rest well my handsome VP SKC
@EmmanuelNtago
2 ай бұрын
Ndpo inenso
@paulphiri-fz9me
2 ай бұрын
❤ love you bro
@PempheroMoleni
2 ай бұрын
Muli NDI ufiti
@chisonimponda363
2 ай бұрын
Vote vote basi
@memorymataka-g7w
2 ай бұрын
Same as me. Ndinkaseka agogo anga akamandiuza zomwe amakumana nazo nthawi ya mcp koma pano sizokuti ndukunva koma kuuona
@GraceZumazuma
2 ай бұрын
Powerful massage father,mwatiyankhulira ndipo chakwera am sure wamva ndipo akudziwa kuti next year zake zada or atatani ndi manganya wakeyo mfiti zokupha zimenezi zikapume
@Geraldmkwewu
2 ай бұрын
Amen amen amve Mr chikangawa fiti
@ANYAMAINGATV
2 ай бұрын
Tiyen tipitilize kuyatsa ma kandulo iziwapweteka daily mpaka kampen wao azakhare opanda mphamvu Amen🙏
@josephinekatupi6919
2 ай бұрын
Zoonadi❤
@TrizaGeorge-q8w
2 ай бұрын
Ndipotu zoonadi ambuye kudziwike kuti kuli mulungu pa ifa ya athu amenewa ikhale panutu Pao ndipo china chake chichitike ndithu ❤❤
@Hellenistic109
2 ай бұрын
Thank You very much Bishop for the Wise Preaching,I Salute You..😢😢😢
@jjhollyland4918
2 ай бұрын
We need this everyday. Men of God come out and preach the truth 🙏
@UsenLashid
2 ай бұрын
Mawu amphavu kulakhula mosaopa munthu koma kowopa mulungu
@Creslevison-vj2sl
2 ай бұрын
Aaaa yes bishop watokota chilungamo uyu eshiii i lv the way he cud articulate the whole story fearlessly amidst mr chikangawa eshiii
@MaxwellChiwaya-tv7kn
2 ай бұрын
Ine mpakana lero sindikumvetsabe kuti Biyeni anamwalira mmmmmmmmm only God knows
@esthermalixani2244
2 ай бұрын
Zoonad
@TonychisalaPhiri
2 ай бұрын
Uthenga usu ngati Chakwera sanawunve pls mutumizileni awunve. Tony Momadi. Johannesburg, RSA.
@NeemaMatewere
2 ай бұрын
Powerful gospel,imfa yowawa ngati ya Yesu Christu,ngati yaa Martini Aku Uganda,ngati yaa Postoli Mtima woyera WA Yesu,mutichire chisoni,a Martini Aku Uganda mutipemphelerw Ife,woyera ose akumwamba mutipemphelere ife. Kuyankhula kulalika zomveka .Amen
@JoyceChaima
2 ай бұрын
Ambuye Mulungu odziwa kuweluza.... aweruze ndithu. MZIMU WA CHILIMA usowetse mtendere aliyense amene anatengako gawo pa infa imeneyi😢😢😢
@EllahChikwatu
2 ай бұрын
Amen 😭😭😭😭😭
@josephinekatupi6919
2 ай бұрын
Amen and Amen🙏
@HappyAnt-uz5je
Ай бұрын
No mtendere mpaka adzafa
@EstherChibwana-lp3gx
2 ай бұрын
Abig message to malawians I salute u bishop
@MirriamChakanza
2 ай бұрын
Powerful message, wakuva wamva. Amen 🙏
@AmosKayira-y1m
2 ай бұрын
Amen, that's why am proud of Catholic bishops! 🙏🙏 may his blood be like those of Martyr RIP SKC
@RuthMasamba-ms2di
2 ай бұрын
Amen and amen, kma2 kudziwike ambuye kt mumatha
@MosesBanda-h4x
2 ай бұрын
Very very powerful , may God continue giving you fearless speeches for Malawians to know the truth of God.
@chinomwephiri1183
2 ай бұрын
Amen, and powerful SKC, may your soul rest in peace
@ifristathope1131
2 ай бұрын
Amen bishop🙏🏿 chatsika blood on his hands. God gonna answer our tears. Osaopa osatopa n osafooka we need better Malawi for all not za sikusinjazi
@LuskaMoses
2 ай бұрын
Ambuye yesu akudakitseni Fathar😢😢😢choonadi chimamasura
I love the Catholics they stand on the truth may God bless you all
@JeanBanda-zy6wu
2 ай бұрын
Osawopa.... kuyankhula koma uku osawanyengelera awa aziuzidwa chilungamo evil people Ambuye achite nanu
@thomasbotha9790
2 ай бұрын
Powerful preaching mau Amphamvu
@vivianmkwate8536
2 ай бұрын
Amen a Bishop tikulira ife Amalawi
@mussamapira801
2 ай бұрын
Mwamvatu a chakwera ngakhale mukubisa umboni anthu akutopelani poti chilungamo nchowawa kuyamba kumanga koma mwa Allah mwini chisoni ndichifundo Ali nafe Ameen mwa Allah
@SangwaniNkosi
2 ай бұрын
Amen mtumiki wamulungu,chilungamo mwanena ndithu
@Extratremendouszeus
2 ай бұрын
Chakwera ndi mbuzi yachabe chabe ..ndichimunthu choipitsitsa pa zolengedwa zonse...matembelero a Mulungu,angero ,komanso onse amene amadziwa kutembelera akhale kwa chakwera oipa kwambiri😏😏😏😏😏
@WisdomPupweeMwalilino
2 ай бұрын
Our God will do it and make us move forward with grace.
@TonyMhone
2 ай бұрын
Amen. Munthu wa Mulungu walalikira mopanda mantha.
@AndsonYusufChiwamba-jw3vl
2 ай бұрын
Powerful message to Malawi 🇲🇼
@gracemkandawire8769
2 ай бұрын
Achita bwino kulankhula ku tchalichi,,atidyenawo akwiya kuteleku,,koma ali mbuu,,
@misoMoyo
2 ай бұрын
Munthu wa mlungu wayankhula mosaopa nae ndi okhumudwa ndi IFA ya bambo Biyeni
@Gwedeza-oz3jv
2 ай бұрын
6:52 Kulankhula mosaopa osati enawa. Amalekeza wakuphayo chigawenga kamba Koti wapatsidwa ndalama , uwu ndiye utsogoleli osati abusa ndi asheikh ena Aja aaa anangoziwikiratu Kuti akugulitsa mawu aMulungu Kwa chikangawa (chakwera) ndi ntengo wotsika mukankhanthidwa patsiku lomaliza ndipo mukasowa kothawila ndalama mubazo sizikakuthandizani chifukwa kuzakhala kulibe,
@GraceMwase
2 ай бұрын
Azibusa ena mzimu ndi mphamvu za Mulungu zinawachokela kalekale angokhala zitsiru kumakalandira ndalama kwa chakwera chigawenga chouma mtima ngati chimenechi chisatana
Пікірлер: 459