Iyiyi nde yandifikapo ndithu big up Hot current 💪💪
@BwanaGD
9 күн бұрын
Tisinthe flag yanthu ilindi mintundu yoyipa ntunduwake mmm ndiwachabe mutundu ya bendera yanthu imagwilitsidwa nthawizabili ndizinthu zakumidima panayenela kuyisintha bas
@Lee-lee-w1r
9 күн бұрын
Koma ndipo Simukunama. Taonani flag ya Kenya 🇰🇪 ndi ya malawi 🇲🇼 sizisiyana kwenikweni koma mmene zinthu zilili ku Kenya ndi kuno nzonvetsa chisoni
@RobertCosmas-bo1uo
8 күн бұрын
Massive analysis this is good idea and solution zoonad katangale akhoza kutha zkufunika azitsogoleri odana ndizopusa that's right guys.
@IshumaelMbewe-d4t
9 күн бұрын
Tidakhala ndi atsogoleri ophunzira angapo koma sitidatukike pa cbuma ndi zitukuko ndiye tidzayese mtsogoleri wa form 4
@PetersenjMwale
9 күн бұрын
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV
@ElizabethMajiga
9 күн бұрын
Apa ponkhapa mwawalakhulila amalawi🎉🎉🎉🎉🎉🎉
@GiftNyirenda-q9d
7 күн бұрын
Koma ma decision makers particularly politicians amamva zimenezi? Uthenga nde ndikwabwino and straight forward. Vuto aliyense angofuna iye ndi abale ake akamachoka, zawo zikhale ziyenda. ie alibe chikondi kwa a malawi koma kuzikonda
@user-mh7cc8up4i
8 күн бұрын
Apankunku ndi ndevi zamwayi mwayamba bho next time muzapose apa apa ndakayika kuti mudadya chikondamoyo we love you lots ❤
@user-sw6rz4tz3z
6 күн бұрын
Suzumilani mu MRA muwone zomwe zikuchitika especially in a hot activities eg boarders kkkk
@PetersenjMwale
9 күн бұрын
U guys u talking the really truth
@SolokingChimzy-yt7dj
6 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂..ati sitidya kwaaaanu eishhhh anyamata anakalowa mu studio ndi mkwiyoo awa...Iman moona mtima ndimopanda mantha ngat Mikaya wa mu Bible yemwe anasutsana ndi mafumu ochuluka pozindikila kut zoyankhula zake ndizo zinali zoona
@blessingsfalamenga4575
6 күн бұрын
Anyamata inu get ready in 2025 boma lina likubwerari tikonze malawi you are good indeed.
@user-em3xq2th4g
20 сағат бұрын
😢 Apa palibezoti bola baja bandani ni same thing those bantu
@louisgolden
9 күн бұрын
Mwauzeso kuti akugulileni track trauser kuti yikhale top and down
@stevephiri1043
8 күн бұрын
Mmoziyi ndamene amalakwisa program amakonda kuwatchinga azinzakewo kuti asamasuke
@dumisanimoyo3152
9 күн бұрын
Amati mwanapiye anawonera make kunyera munyumba nde tiphe mayi wakeyooooo
@lastonmasoatenganji-bs5gf
7 күн бұрын
Tikadali njira, sindazione munthu wa zaka 60 akukakamira kuyamwa bere la amache. Mkakawo udakoma chotani.
@ChettoSongeah
6 күн бұрын
impressive guys Ndevu za mwai umaitha ndi nzako yo 🤞
@Erickasonya-uw8yw
6 күн бұрын
Bravo guys mumakwana
@kotking-xg7pp
9 күн бұрын
MWALANKHULATU MWAMPHAMVU RELO NDIYAMIKE KWAMBIRI.
@clintonhodda9830
9 күн бұрын
Koma a Brown mpinganjira mpaka liti osavomeleza kuti Mulungu sanafune kuti akhale president iiiii
@HastingsJonathan
8 күн бұрын
Nelson Nelson 🤣🤣ukumaika ma flash et
@jelsonmlowoka8611
9 күн бұрын
Zoti inali times television yooneledwa ndi anthu ambiri pano ndi history chabe hahaha ndaonela ma viewers ndi kuchuluka kwa ndemanga
@EdwinMakwangwala
9 күн бұрын
Ambiri amaonela but they reserve their comments but ndawakonda ma guys
@user-em3xq2th4g
20 сағат бұрын
❤😂😢 nkhani yagona pa utsogoleli, kwa anthu amene ukuvoteledwao, tinawavotela pachifukwa chiani?😢 Kd tinawavotela chifukwa choti mwaiwo tikuonamo muzimu wa utsogoleli? Kapena chifukwa choti tikumadyanawo? Apa tiwonepo apa, kwa Ife ngati ovota. Kwa iwo amene akhalapo atsogoleli, ndi iwo amene ali atsogoleli, Asanapange chiganizo chofuna kukhala mtsogoleli anayamba azifufuza okha kuti mwaiwo yilimo mphatso ya utsogoleli kapena ayi? Akulu akulu tisaname apa onse amene tawavotela awa ndi amene tikuwavotela awa akungogweramo chifukwa chokakamizidwa ndi anthu ane amene ali atidyenawo, chifukwa cha mzimu uwu uwu, woti tikamuona munthu ndikumuwuza kuti km inuyo kuti mukhale mtsogoleli anthu akhoza kukuvotelani zaziiii, mawa olira ndifetomwe, muMalawi alimo anthu anzelu ophunzira aliso ndi utsogoleli mkatimwao km chifukwa choti ndi osauka palibe munthu amene angawa votele, pano ndi izi zaka 60+ chifukwa chokonda kusankha bakawalala aba tilindicha zero chosangalasa ndichani kumuvotela munthu maba akukufiya pahoroh 😂 kpn kukumanga ndikukakusekera inside kirikiri😮
@nellybruhan5834
9 күн бұрын
Ine nde kumalawi kwandikwana😭😭😭😭😭😭 thupi lonse likumachita kuwawa ndikuganiza
@user-ec3xh4pc6t
9 күн бұрын
Dear bwelani mbalikuno bas
@nellybruhan5834
9 күн бұрын
@@user-ec3xh4pc6t kutiko kumeneko saka bag yanga ndapakililatu
Malawi has suffered leaders who kept us in the dark for years. Without water. Leaders that store n cut all rail lines to replace it with mangochi based vehicles. The nation suffered from leaders without teeth who paralized universities for almost a year. If asked, they would go on holiday in the USA. Now, are we promoting such leaders to come back? This is an opposition forum. Not a program that talks reality. None bias reporting is what this nation needs.
@OssmanAbubaker-l5s
5 күн бұрын
Zoonadi my brothers osaopa osapepesa zaka 4 palibe chanzeru olo chimodzi chimene achita awa a Tonse
@GraceZumazuma
9 күн бұрын
Keep it up times musalore akupatseni ma banz mudzitiimilira chonchi
@dysonmasiye5736
8 күн бұрын
Za katangalezi tinaluza munthu wofunikira kwambiri amene anali ndi masomphenya pa nkhani iyi....SKC 😢 tidzamlila mpaka kale...koma adaferanji?
@gracemkandawire8769
8 күн бұрын
Brian alikuti Kodi? Amabebetsa
@christophermukaka7403
6 күн бұрын
To say the fact ma guys awawa amayankhula zoona koma kumtunda ku mmm
@sparkdymon3429
9 күн бұрын
Iyi koma mwang,alulandi makosana abwana kutundako azizifusa makamaka achekwela ndimbava ndifukwa akopa ACB
@user-ux8bc6wy1i
8 күн бұрын
Iyi ndye hot current yen yen 🔥🔥🔥
@mustafahassan9128
7 күн бұрын
Koma ndiye mwanena mosanyengeleratu
@user-to5of3ks3g
9 күн бұрын
Nice message
@obviouskedson6483
9 күн бұрын
Ife timamva nanu kukoma chifukwa mumayankhula chilungamo ,ndipo nthawi ya program yanuyo muionjezele mabwana
@user-sw6rz4tz3z
6 күн бұрын
Musogoleri akawoneka wa good future kumapha basi
@user-pv9uk6sc3w
9 күн бұрын
Yeah! This is hot for sure.
@user-si7po9sd5i
9 күн бұрын
The curtain in the temple is about to be torn, we are waiting eagerly
@EdwinMakwangwala
9 күн бұрын
The problem of you and us as Malawians we always celebrate when someone fail, this is very bad and ugly kkkkkk
@user-si7po9sd5i
9 күн бұрын
Sometimes it's good to understand the message properly,who is celebrating here? If someone is failing to run the affairs of the country,how does that concern me?,he has 23 advisors,What is their job?what are all the advisors doing, this is high level filth,Justice hurts.
@Lee-lee-w1r
9 күн бұрын
@@user-si7po9sd5iexactly tell this person the truth
@Lee-lee-w1r
9 күн бұрын
@@EdwinMakwangwalait’s not celebrating them. It’s celebration that the truth about them will be coming out
That's why they assassinated malemu mnyamata woganiza boo Adamupha KS and they think we have mastered the crime and they will not be able to be caught and arrested.
@augrinngunga8031
8 күн бұрын
Mwalakhulako zazerutu, mukamadya ma bazi guys times izakhala Ngati MBC yoonera achakwera okha
Пікірлер: 123