Your the first guy I see ur praying on social media before u start ur program God will lift u my brother and don't be shaken
@chisonimponda363
2 күн бұрын
Ndipo great n awesome guy
@AdamAhamad-k2i
3 күн бұрын
You're a hello my brother may Almighty God protect you from evil people especially MCP members
@MemoryAllan
3 күн бұрын
God loves people who speaks reality,my Allah protect you all days
@Dickies-mk8cd
3 күн бұрын
Any weapon formed against you will never prosper Mr A Kamangila.
@BrandinaMphuka
3 күн бұрын
Ayamba kusaka akatero asowetsa ndukufunira chitetezo mudzina la yesu Nazarete amen
@AchimkokoChigonambango
2 күн бұрын
Akudziwa zonsezi Pali ma galimoto awiri akusinthana ma shift kumamusata, he knows it all
@BrandinaMphuka
2 күн бұрын
Mmmmmh koma abale dziko lapansi limadana ndi chilungamo koma sizitheka
@Yungjoe786
2 күн бұрын
This guy needs support,we’re sick & tired of our useless politicians for sure
@ChimwemweKondowe-nj4lx
3 күн бұрын
We need people like you in our generation
@MrsNankhumwa
3 күн бұрын
God protect you brother, muli cha uzimu mkat mwanu amwene,mumaopa Mulungu nchifukwa mukuima pa choonad, Mulungu akulitse malire amoyo wanu
@alexsumani6823
3 күн бұрын
kung'alulidwa, very courageous man Malawi need people of his Calibre
@jamesmoyo6914
2 күн бұрын
Our those guys let’s be with him
@andrewmwanza5696
2 күн бұрын
This lawyer has said it ALL. A Malawi ambiri omwe anavulala pa ngozi zapamseu, amangodyeredwa ma compensation awo. Judicial system in Malawi is so rotten. Kudos to you lawyer.
@peterbakuwo1249
3 күн бұрын
A new king in the ring... Kasongo eehya,eehy Kasongo aaeee! Carry on brave man..! No fear,
@EsnartGirivin
3 күн бұрын
Chilungamo chiyende ngati magazi a Yesu nkhristu❤
@isaackapenuka
23 сағат бұрын
God protect you, this is what we're looking for bravo!!!!!!
@andrewmwanza5696
2 күн бұрын
This lawyer is the best I have ever heard. His integrity is equal to that of white people. Not common in Malawi.
@MaganizoKaloza
2 күн бұрын
You are a true Malawian.Who soever may think to destroy your life will not succeed..Amen
@Mobilot2android
2 күн бұрын
Iwe ndi Dolo ada ndipo umatha kuchedza... Ndipo machedza aiwe anthu azibibila nzikomuno May God bless you Bravo and long live
@KondwaniLungu-x5l
3 күн бұрын
Mulungu wakwiya nalo ndi zikoli ndi anthu oipa kuntundaku that's why aku user munthu ngati ameneyu. Ichi nchiyambi chabe , nkwiyo wa Mulungu ndi owopsya ine i feel's kuti nthawi yakwana wayamba kuwalanga izi ndaziona pa ka time sure kulira kwa amphawi Mulungu amakhala nayo serious and likakwana la 40 ndimmene zililimu , coz sizophweka wagulu lawo kuima pachulu chonchi , apa pokha guys Mulungu amatikonda kwambili.
@EmmanuelGasiten-fo5dr
2 күн бұрын
You are lyk King Solomon. Bravo bravo bravo
@Nelsonmatenda
3 күн бұрын
You are the greatest man indeed of malawi
@JustinLipipa
3 күн бұрын
Your a good Man, God provide our country with only 10 fearless people who are in better positions so that they can speak on behalf of us poor people. God bless Mr kamangila and others who are contributing evidence about Corruption.
@Sabina-hw4js
3 күн бұрын
We wonder why malawi is poor,it makes me angry too.
@WilliamMajiwa
2 күн бұрын
May Almighty God protect you from All your enemies and bless you abundantly.
@MarySelenje
2 күн бұрын
Bravo! Bravo!! Bravo!!! Bravo!!!! Bravo!!!!! God Almighty will protect you accordingly Mr Alexious Kamangila.
@FixsonMkwamba
2 күн бұрын
God bless you ALEXIOUS. Protect him from the evil dowers.
@ALEXAlli-ck8lj
Күн бұрын
A katundu mr kamangila big up
@mzeewandembonyirongo2972
3 күн бұрын
I have listened to end. And you are determined and seems you know what is happening in your sector. And you have mentioned names...let them sue...and you will give evidence. You are aa great counsel...may God protect you..❤
@P.Bilali
3 күн бұрын
The guy needs support
@chimwemwefrighton4080
3 күн бұрын
Next Chief Justice to come...
@evanszgambo4009
3 күн бұрын
More Blessings upon you ,This is a wake up call
@Sabina-hw4js
3 күн бұрын
We need God fearing people like you
@georgesmart3791
3 күн бұрын
Well said mr... you are such a hero❤❤❤
@JimmyMaster-l1x
2 күн бұрын
In the Name of Jesus Christ sizitheka kt akusowese brother
@billykhoviwa6616
6 сағат бұрын
big up bro....our own Ibrahim Traore
@SifatiMoses
3 күн бұрын
Mulungu akhare nanu nthawi zonse, anthu monga awa ndi omwe amafunika dziko. Paja boma lina limadana ndi anthu onena chilungamo koma apa pokha simudutsapo. Ndipo kungosowa munthu uyu tikuocha nyumba zanu live.
@corretabanda7685
2 күн бұрын
Jesus said muli ndi tsoka inu afalisi ndipo sanawope kuwadzudzula, koma anadananaye koopsa. Ambuye mtetezeni mwana wanu chifukwa ife tikudziwa kuti ndinuyo mukuyankhula kudzela mwa iye.
@Sabina-hw4js
3 күн бұрын
When you fear God you do not fear to say the truth
@Sabina-hw4js
3 күн бұрын
Then the president just looks at this!!!!and calls him self a Reverend!!!!God forbid
@WonderfulChibisa
3 күн бұрын
Ndimbuli pa nkhanizi m not surprised
@YoungMwacho
2 күн бұрын
Iyeso ndiwakuba ayankhula chani?
@KondwaniLungu-x5l
3 күн бұрын
Wishing you all the best maybe some others can change they are mindset, vuto ambili akakhala kuti ndi ma judges amaona kuti palibe aliese angawatutumuse ndie amangopanga za miss behavior zosamva chisoni 1 ndi ziko lawolomwe kumali ya anthu omwelawa pena kumukhomelera munthu amene amaenela kuti a wine mlandu.
@babranzima8120
3 күн бұрын
God protect you mr❤❤❤❤
@BerthaMATUMBO
2 күн бұрын
Good work brother may God Almighty bless you
@wisdomsadyalunda2001
2 күн бұрын
The strength of the evil is in our fear.. This is powerful.bro..
@yasiniKalonga
2 күн бұрын
Zinakat wakufa amadzuka kumanda bwezi ndikt uyuyu ndi kasambala 😂😂😂😂more fire 🔥🔥
@JosephyMakunganya
3 күн бұрын
Anakadziwa ku CHANCO ko uyu anakamu wida 😂😅 But its too late Broh continue 💪🔥.
@user-ux3ed3ni1p
2 күн бұрын
We are with you all the way. God bless Malawi 🇲🇼 and its people. We have suffered enough.
@mzeewandembonyirongo2972
3 күн бұрын
This counsel mmmh has stories.... JUDICIARY wakeup call
@DavidPhiri-o6w
2 күн бұрын
My hero, lawyer kamangila
@mkandawirem610
3 күн бұрын
People like you amasowa boss, very important things to know as Malawian
@KondwaniLungu-x5l
3 күн бұрын
Even malemu kasambala I don't think kuti anali judge wachisanzo chabwino. So iwe utha kukhala oyamba enawo kuima pachilungamo ku gulu , Mulungu apitilize kukuthandizila pa ichi.
@YoungMwacho
3 күн бұрын
This guy is loves Malawians and is ready to die for them. May God protect you bwana.
@KondwaniLungu-x5l
3 күн бұрын
Mulungu wakwiya nalo ndi zikoli ndi anthu oipa kuntundaku that's why aku user munthu ngati ameneyu. Ichi nchiyambi chabe , nkwiyo wa Mulungu ndi owopsya ine i feel's kuti nthawi yakwana wayamba kuwalanga .
@RobsaiSaidi
2 күн бұрын
This guy is very good... keep on opening our eyes to see zobisikazo
@emmanuelalbertbotolo
3 күн бұрын
❤❤❤❤❤❤❤very good brother u do good and noone scared you, God is ur side all the time
@MarryNyilongo-s5x
2 күн бұрын
You are an angel
@shayrafernandeslatif9556
3 күн бұрын
Ine ndaziwoona ma cases anga it's been years kumango phiphiristidwa
@Blessings-td4cr
3 күн бұрын
Big up bro,,,we will just keep you in prayers coz zamalamulo mbulife sitikuzidziwa koma timenyereni nkhondo kuti tikadzapalamula tidzapeze chilungamo pamawa ,,that's good nowadays kuima pa chilungamo.
@WillyNyirenda-l7h
3 күн бұрын
Judicially needs overhauling and time is now.
@HerbertTchautchau
3 күн бұрын
Morepowerfull word go Aheard Big
@AgnessChapinga
2 күн бұрын
Ambuye mwanayu mumuteteze ,Adani apapa mitu sikugwila
@serakillo8668
2 күн бұрын
Your ❤❤❤❤ keep it countinue good work my brother
@patrickmatabwa5828
3 күн бұрын
May the mercies and protection of the good Lord be with you...
@MorrisMapiri-o4k
3 күн бұрын
If justice is reformed, everything is sorted.
@AbrahamLLoyd-xb2xc
2 күн бұрын
Keep it up brother
@samanthamuller7643
3 күн бұрын
I love you ❤❤❤❤ man I need like Malawian
@LawrenceMalinda
2 күн бұрын
Keep it up my brother , may God protect you
@TimeAbilu
3 күн бұрын
Keep it up my brother your the first one and Allah bless you all the time
@ChomboNgosi
3 күн бұрын
God protect you always
@StuartGondwe-n5j
3 күн бұрын
Ziulure mbuzi zomwe zikuononga Malawi.
@SherryJiya-c1u
3 күн бұрын
Ibrahim traore waku Malawi...mulungu watumiza uyu
@Sabina-hw4js
3 күн бұрын
You are a hero
@JacklineNiwahereza-ni3pm
3 күн бұрын
Anaa mumalawi ali ndikuthekela kosontha zinthu
@abudullraheem
3 күн бұрын
We need to build our national ❤❤🎉
@ajasikalonga3210
3 күн бұрын
God be with you my brother
@FrancisMalunga-g1j
3 күн бұрын
Apa nde wabudula mpunga wagulutu mkuluyu 😂😂😂
@YoungMwacho
2 күн бұрын
Nkhani ya Kayuni anatumidwa ndi Chakwela, an evil Pastor, mbava yopanda manyazi.
@MayamikoYMsusa
3 күн бұрын
Koma mwana uyu,,mulungu amuteteze
@PhyllisMambo
2 күн бұрын
Iwe ndi uja olonjedwa uja amene timamudikira ulemu wako Kamangira God is in your side and we are playing for you
@juniortsegula3847
3 күн бұрын
We are praying for u brother. God protect u
@JacklineNiwahereza-ni3pm
3 күн бұрын
Thus is gez generation he born in 1998 young leaders first we are tired of these old people
@RobertLuka-wy9cl
3 күн бұрын
God bless mr❤❤
@AnnieMpenda-vx5wb
2 күн бұрын
In Christ Jesus you're protected and covered by the blood of Jesus Christ 🙏🙏
@jacquelinChitsulo
3 күн бұрын
Kugwiritsa ntchito mphanvu kulanda katundu wa eni
@Uladimbwana-fr9ev
2 күн бұрын
Chakwera himself have to be investigated
@JalitahKatumbu
Күн бұрын
I will stand with you
@AmosBandula-up4yb
2 күн бұрын
GOD bless you my brother
@RosinaPatel
2 күн бұрын
May the Almighty God protect you
@Fatima-db8ut
2 күн бұрын
Psalms 91 verse 7 over Mr Kamangira
@MacdavieIteta
2 күн бұрын
Anthu ofunikira mdziko muno ndinu bwana you are our next president of tomorrow me konda you big
@BirzetScott
2 күн бұрын
❤❤ God protect you all the time
@SophieKabango-b7p
3 күн бұрын
Include the case of Greenlight Investment whose accounts were frozen since March/April, 2021
@MickdadSaiti-mj7vi
2 күн бұрын
Koma mukazamupha uyu, kuzavuta
@banyakolemulenga7072
3 күн бұрын
Hope you were in Zambia
@EmilyKanyika
3 күн бұрын
❤❤❤❤❤❤❤
@Sabina-hw4js
3 күн бұрын
We are praying for you
@GrecianWyson
3 күн бұрын
Komaso mlandu uja wa chisakho 2019to2020 sunayende bwino oloko.chigemuro Choti kaphatikizaneni mmala Moti aliyese ayime payekha eeeeee INE zinandiwawatu esh Mulungu yekha basi
@Uladimbwana-fr9ev
2 күн бұрын
Koma iweyo mulungu akudalise ndinthu, let's wake up this is a time mulandu wakuba nkhuku 15yrs mulandu wakupha munthu kumayenda mwa umfulu
Olo mulandu wa Bakili muluzi umatha chonchija kdi milandu yaikulu ngati imeneija, kutha mwachidule chonchija kdi zikupeleka picture yanji kuziko? Ine izi sizinandisangalase konse milandu osokoneza chuma cha ziko and mapeto ake milandu nkumatha chonchi si zoona. Mapeto ake zikoli lisauka koopsya, why kuntundaku aziononga ndikumati azandikhulukila what's that.
@Sabina-hw4js
3 күн бұрын
To be a judge is a calling so u need to be honest
@AnnieMpenda-vx5wb
2 күн бұрын
May God help us,ma judge aku Malawi all are corrupt. Amakondera anthu Ali ndi ndalama. Samafuna kumba voice ya odandaula akakhala kuti odandaulayo alibe ndalama 🤔🤔🤔
Пікірлер: 162