Ndipo apolisi amanyi nonse mukonzeke pa ten pano tikaphane basi oyamba kufa sindikhala ine ndatopa nazo mungosekelala zopsa basi kandalama kake kati komwe mukugulisila anthu osalakwa
@joyahmedjoma4615
2 күн бұрын
Big up Mr bon kalindo we president 🎉🎉🎉❤❤❤❤zikuntha pa 10 zimenezo za maminazo apampa tipanga za ku kenya 🇰🇪 pa 10 si patali ai so soon ife amalawi ndife wokwiya ndi boma la chakwera never go back
@user-wu8kp7ui5j
2 күн бұрын
The DC 🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@ChimwemweKondowe-nj4lx
2 күн бұрын
Very true The great Bon Kalindo. Opposition need to go and challenge this new rule of no 🆔 no voting. Otherwise, we don't need NRB in our country because they're working for MCP and not Malawians
@lameckmajiga5426
2 күн бұрын
Muziko mwanthu muno mukuchitika zinthu zonyasa kwambili koma ife anthu timawopa kuphedwa kapena kumangidwa!!! Ili ndi ziko la democracy not one matparty system
Panopa ine ndikupanga biziness koma profit ndiyaying'ono kwambiri. Mutu wanga wayima.
@user-pf5hu2pd2b
2 күн бұрын
Chakwela ndi mbutuma yamunthu ndi gulu lake
@user-nf3ik3ff6y
2 күн бұрын
Good Messnge my Bon Kalindo
@johnnyeliah4302
2 күн бұрын
That's true Mr. D.C
@thomasbodo4099
2 күн бұрын
Boma la anthu opusa ma savage
@BashiluChimake
2 күн бұрын
Ife2 tikudikila ndodo ituluke
@FrankFrancis-ch3xv
2 күн бұрын
Yes!kodi izatuluka liti ndodo
@user-po6ir6eh4z
2 күн бұрын
Dc muchita bwino nkhani ma ID muitengere ku court ndikutheka a opposition anaphwisiridwa ndi agule mulumusan malawi. Ponda anthu angati unu ziko lathu likafera ku banga moyo
@user-ul1fb4yn5o
2 күн бұрын
The DC mwana woooopsa kwambiri
@MarthaJafali
2 күн бұрын
Vuto lovotela mulimi ndi kupanga president ndi limenelo munthu wakukakasiya ndikukukhala president manthongo Ali tho azasukusula liti
@user-jw5rx9ze8k
2 күн бұрын
Olo uyankhule mbwelera, timamukondabe The DC.
@MisheckSenga-q4i
2 күн бұрын
Mmakwana boss mn
@ChrifordBiziel
2 күн бұрын
Akuluwa akufuna kusochelesa anthu iwowa akudana ndikusakhara pa udindotu
@lameckmajiga5426
2 күн бұрын
Akulu inu pamutu panu sipakuyenda bwino!! The D.C is only man come on public and tell the president true!! Ifetu tili kumbuyo kwa kalindo ndipo inu a MCP musanyengeke kuti mukalowa ku 2025 otherwise third-wool ija izayambika!!
@PatrickSamson-po7uy
Күн бұрын
Umakwana
@VictoriaWilly
2 күн бұрын
Munthu wamkulu zedi, the DC
@dontreybanda278
2 күн бұрын
Good massage boss
@McshonWilliam
2 күн бұрын
Mashing opangila mashin anzake D. C NUFF RESPECT TO YOU MUMATIIMILIRA 💯💯💯
@DanNzima
2 күн бұрын
The DC!!!!
@MarthaJafali
2 күн бұрын
Ndipo inu a China pharaoh amenewa Sali bwino mulungu wa Israel awayendele
@miraclekayira9613
2 күн бұрын
Kalindo...The Great Man....winawe osangochoka bwanji
@BENSONRANGWANI
2 күн бұрын
Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach
@Enock-c9l
2 күн бұрын
A opposition afasa ngati Chilima
@user-fi7ko7bl6f
2 күн бұрын
The DC chimwana cholimba mtima kwa osauka more 🔥🔥 Mr Kalindo Tell them😅😅
@hanifahmponda8711
2 күн бұрын
The DC koma otsusa akudziwa chilichotse chimene aboma koma ndele ndidzimenedzo akufuna aboma adziwona ngati zawo dziyenda chifukwa chachinyengo chomwe NRP ikupanga pa kalembela wa ma ID muthalika chihana atupele mayi patelo ndi akaluwa ndianthu oti angalole DZOPUTSA ZA ID ALEMBANA CHIGAWO CHAPAKATI CHOKHA AAAA AKADZALENGEDZA KUTI ALEMBETSA VOTE NDI AMENE ALI NDI MA ID WOKHA NDIPAMENE AMALAWI OTSE KUMWELA KUPOTO DZIWONETSELO PAKA PAKA TIZAVOTE NGATI MBUYOMU ADZATSINTHE NDIPAMENE TIDZASIYE KUMANTCHA KUPANDA APO CHITSANGO KUDZAKHALA KULIBE KOMA CHAKWELA NDI MCP YAKEYO ADZACHOKA PAPANDO ASATITENGA NGATI AMALAWI DZISILU CHAKWELA NDI MCP AYAKOYO NDINU AGALU KWABASI
@Leo-fj6gz
Күн бұрын
The Dc 👹👹👹👹
@GiftPhiri-tt7nn
2 күн бұрын
Pa ten wa police wamakani tikaonetsana ,apolice mumakhala ngati inuyo kut mukugula sugar 5hundred pomwe tonse tikuvutika limodzi ndiye mukachuluka nzeru pa ten muluza miyoyo ovutika akhala abale anu , and mufera zaini chuma akudya mabwana anu inu okathira tear gas pansewu ,muzuzutsa abale anu ndi ana .
@Extratremendouszeus
2 күн бұрын
Nde nkhani zake
@SolomonNjolomole
2 күн бұрын
Audio iyi yandikhudza kwambiri.
@user-ty4pq5ub3q
2 күн бұрын
The DC. Chimwana choopsa kwambiri ..ine buzines wanga anaduka kale kale.
@LazarusEvasonchafachaola
2 күн бұрын
D.C ukhalise umatiimilila kwambil
@Pangolinimw
2 күн бұрын
The DC
@GiftKananji
2 күн бұрын
Timakunyadiran bg
@user-ji4xn6me8d
Күн бұрын
Indeed it's bullshit a MRA the DC ayankhula
@user-gj4li2gc8o
2 күн бұрын
Munthu ukuzitama wekha iwe ndiwe chitsiru chenchen
@ZionekaMember
2 күн бұрын
Iwetu akupasazo ukabweza
@dalitson3558
2 күн бұрын
Chitsiru ndi wagule akulephela kuyendesa dzikoli, kwacha kumangogwa siku ndi siku
@clintonhodda9830
2 күн бұрын
The DC mwana olimba mtima
@rachidecaundealy8335
Күн бұрын
Assani,keti
@EllenPhiri-xt8pt
2 күн бұрын
Wenawe ngati wadya ndalama za eni tuluka usamanvele apa ife ndi bon ❤ wagwana nayo pita ukabweze ndalamazo cos apa walephela 😂😂😂😂😂😂
Пікірлер: 106