Izi mukunama Boma la Nankhono Lili Bali iti yadziko la Malawi.Mwazi wa chilima ukukuzuzani mupenga tikuonelani.Bakili tv Komaso Limpopo FM ilipo ikutiuza zonse.Mokulemekezani bwana mukunama kwambiri.
@augustMag
5 күн бұрын
Mmmmmhu ndiye nkhani mutu wake ndi chani?
@PatienceMphuche
5 күн бұрын
Kkkkk koma anthu atopatu
@user-uc1pd1tc2x
5 күн бұрын
Pls ndiphwanyiredi Chakwerayo ndi Zikhale Ng'omayo Komanso Kunkuyu pls pls
@user-rg4du4vu9r
5 күн бұрын
Kkkkkkkkk km wina akango khuta bonya wake uko basi wapeka zakezo nkumaza rankhura apa km zina zot usagura kunvesera kumat awa akuchita kunveka kt nyumba mwawo ufa muribetu awa kkklkkkkk nazoni guys 😂😂😂
Пікірлер: 44