SKC was a general fitter analibe kuyankhula za munthu koma maso ake anali ku dziko la malawi kuti lizakhare pabwino, now Usi amayenera kuwafikira a U TM amnzake powawuza za kusankhidwa kwake
@GeraldMkwewu-gd5eb
5 күн бұрын
Chitsiru manganya ndiwa MCp anampha chilima ameneyo anakambapo Chan Za lfa yachilima galu uyo ndi chakwera
@princedetbozsmallboy1749
5 күн бұрын
Tikudabwa nawo anthu ena usiyu anaphanawo Chilima shame on him galu
@jelsonmlowoka8611
5 күн бұрын
Usova iwe ndiwe ndani kumuletsa usi kusakhala vp wa dziko, why did the utm owner appoint him as his runningmate at first, leaving you with no any position in the party?
@GibsonBanda-ey2gc
5 күн бұрын
umbuli
@AckimMhango-v1x
5 күн бұрын
Vuto lalikulu ndi boma chifukwa linayamba kukhala ndi Usi before Chilima asanamwalile
@yohaneben5452
5 күн бұрын
I think most of the people don't know more about usi,although he is vp of UTM but originally he is a member of MCP.
@user-ui7wv1mb4g
5 күн бұрын
No need for imposing Usi on UTM. Usi has been so slippery in UTM. Let him go and we shall see if he is going to survive in MCP. UTM Executive may opt to accomodate him but as for ordinary members its a big NO! Why this time? Where was he all that time when our dear president was alive? Zachibwana a ayi. Usi safunika. Apite akachite zake aone ngati angadzatione.
@StewartMustafa
4 күн бұрын
Yes Usi can't survive in MCP if he doesn't know. But let's give him chance to proof him self whether he z an UTM member or not?
@DysonKamama-yh7hq
5 күн бұрын
Zitheka bwanji munthu anzako akulila koma osakakumana ndiakuchipani chanu before kulumbilisidwa, iye nkumakasangalala chilipo
@CharityChikomo-hl1gz
5 күн бұрын
My question exactly was he never suppose to ask his fellow utm members before making his mind???anywy zoona zidzaziwika mu nthawi yamulungu
@PociahMack
5 күн бұрын
@@CharityChikomo-hl1gz zimene a mayakhula a UTM munthu amene anali ndi umunthu kunali kovuta kumakhala nawo, even akubanja paja anatulusa chikalata chowadzudzula.
@user-ko2yv4gi5y
5 күн бұрын
Chilungamo ndi amanganya anatengapo gawo lakuphedwa kwa saulosi chilima ndingakhale pakwanu pa inu mukuyakhula pali munthu amene anatenga nawo chigawo kuwapasa udindo iwowo kulibe kathu koma chilungamo anthu aku utm akudziwa kuti panali ngwilizano pakati pa manganya ndi chilima
@user-xz7mo8zy8f
5 күн бұрын
Cheap propaganda. UTM mukuganiza bwino kwabasi
@RonicSouza-sk5ux
5 күн бұрын
Usi didn't consult the party when he was told about the news of his presidency
@leonardzchavula3139
5 күн бұрын
Its unfortunate that UTM has not shown any excitement on the appointment of Dr M B Usi,however constitutionally he was the appropriate choice.Had Chilima won the presidency in 2019 Usi was to be State Vice President. UTM has just to accept the situation.
@actuarialscience2283
5 күн бұрын
I am on one of MCP whatsapp groups. I know that Usi is MCP. I am also an MCP member but I don't like Chakwera
@MirriamKambale
5 күн бұрын
He deserve deserve the appointment coz he was utm vp but it doesn't mean utm could have been overjoyed coz they're still in mourning time
@Betty-fe9ql
5 күн бұрын
His conduct from the 10th leaves a lot to be desired, your senior dies and you don't say a single word what's that
Kusankhidwa kwa Michael usi wasatila ndondomeko yake chifukwa iye anali osatila wa the late SKC.komano tingodziwa kuti usi ali ku UTM kapena ali ku mcp?
@user-un6qv6sj3h
5 күн бұрын
Adalowa kalekle MCP
@user-ik5sz8hc6f
5 күн бұрын
@@user-un6qv6sj3h vuto ndilimenelo.Anayenela kukhalabe wa UTM kuti alemekeze ukuru former president of UTM
@isaihmagani5697
5 күн бұрын
Nonse ndinu wanzeru zochepa mulankhuranu a UTM atiuzeso chani poyera zaku lephera kwao kosapezeka kolumbilitsa, pomwe anjawala adanena kale tikadalira nde mufuna atiuzeso chani za milandu basi
@GraceZumazuma
5 күн бұрын
Koma anthu Inu muli ndi nzeru?a utm apita bwanji kukaombela mmanja ali pa maliro?Kodi malamulo ake amtundu wanji week sinathe ena ayamba ukuvina kulumbilitsana a Malawi?which means it was planned this b4 imfa ya chilima khalani ndi nzimu waumunthu eeti
@HalisonSolomon
5 күн бұрын
Nonse munakonza program iyi ndinu anthu opanda nzeru mukuonesakuti muli mbali ya mcp mumafuna kuti a utm akapeze ku parliament chosecho president wao wangoikidwa kumene m'manda, athaphedwa ndi mcp agalu kwabasi zikanakhala kuti zachitika mnyumba mwanu sibwezi mukukamba uchisiru mukukamba apau anthu opusa opanda chisoni
@user-un6qv6sj3h
5 күн бұрын
True bro
@rodgerskatengeza1903
5 күн бұрын
Constitution imapeleka masiku ochepa president or vice president akamwalira kuti asankhe wina
@mathewssimbi3052
5 күн бұрын
Koma ngakhale palibe umboni okwanira mafedwe a chilima ndiwonkhumudwitsa kwambiri ndipo ndiwokayikitsa kotero mkovuta Kuti lero ndi lero akulu akulu a UTM adzikapezeka akuyimba nthungululu pamwambo wosankhidwa Kwa Ausi kotero kusapita kwao kumwamboku mkovetsetseka zongofunika tsopano kuwona kutsogolo
@hagayichiluwe
5 күн бұрын
It's just reminding me that sanje kapena nkhwidzi exist
@CHIFUNDOCHINA-lp9lg
5 күн бұрын
Vuto la USI anazionetsera KUTI Sali ku UTM,ATANGOMWALIRA CHILIMA,Nde chipani chisangalala bwanji
Ngati palakwika kulumbilitsa a Usi nsanga ,tilolerane inuyo mukudzidzulanu sindinu angwiro muli ndi zofooka zanu choncho ngati late Chilima adasankha a Usi adaona kuthekera komwe kuli mmenemo. Kaya wina afune kaya asafune zili choncho basi olo mutukwana olo mutakhala chete ,zichitika zomwe mulungu wavomereza
@user-nj5vu8cd5l
5 күн бұрын
This is talking reality... Kodi ndani sakuziwa ngozi vuto ndilakuti ndi ndege yoyamba kugwa ku Malawi. Komaso DPP yokusonkheza moto kwambiri kuti utm isokonekere
@princekandulu4542
5 күн бұрын
Mmenenso MCP n imakokomeza mikangano ku Dpp
@chimwemwedulla6760
5 күн бұрын
Ndiwe mbuzi
@spargomw
5 күн бұрын
Mwana wa Ng'ona iwe, khakhakha. Za DPP zikukukhudxa chaaa, zipangan zanu. Ife tili ku ma stand
@user-mz8nw6nx6p
5 күн бұрын
Malamulo amanena kuti for 7days pasankhidwe munthu wina,,komaso sakanankhidwa wina koma Usi chifukwa anali vp wa chipani cha UTM,,so guys I don't know why we don't understand for this issues,,,we suppose to understanding because it's a rule,, it's not opinion for someone
@GeraldMkwewu-gd5eb
5 күн бұрын
Inuso mphokoso kusowa zakamba position ndikuluza munthu malamuro ndichani zachamba et manganya amafuna Kare uvp Kare that way anamupereka chilima kwa mikangoyo mukusokosa kusowa zakamba
@user-ez4ru5sk2l
5 күн бұрын
The truth is that SKC shoes are unfittable in all the alliance...and entire country leadership currently....but the country has to move forward.....ndale sizinthu zamuyaya ... it's about servanthood ... service to the people
@tamalangoma2765
5 күн бұрын
May be you should blame late VP for choosing Usi ngati VP wake. Please stop making too much noise.
@chimwemwedulla6760
5 күн бұрын
What noise achitsiru inu
@user-hl3st3cc4v
5 күн бұрын
Koma tu anthu mcp mukamapanga zithu mudziziwa kuti mawa ndi tsiku Lina
@sarahmphande6108
2 күн бұрын
Onse Ali apa ndi zitsilu , how Catherine be sitting and talking while the responders they say ,they are still mourning and it's true Malawian are mourning ndale zophana basi achewa opanda Pache inu
@user-ux3ed3ni1p
5 күн бұрын
What is Dr. Usi bringing to the leadership of VP and UTM. will be the question.
@user-nj5vu8cd5l
5 күн бұрын
UTM this is your good time and best Future be united guys chipani chizalowa muboma pachokha don't expect kuzalamulira Malawi
@ishmaelsiffah9900
5 күн бұрын
Ussi samapanga za UTM n the sad point ndizomwe timaziona munthawi yomwe anthu amapanga zamaliro a SKC ndi ena,iwo aja being munthu wamkulu wachipani pambuyo pakumwalira kwa achilima iwowo ndamene timayembekezera kuti ndiomwe azititonthoza ndikumatipatsa ma update amomwe tiyendere koma mmalo mwake anamusiira mzimai kumapanga zazimenezo n zinatengera kulimba mtima kwamai Kaliyati osatopa,osafooka kumatiyankhula amalawi nthawi ndinthawi,mukumbukirenso kuti ndi a Ussi omweo akuwafunsa zakuimila kwao kwaku Blantyre anakanitsitsa kutchula kuti akaimila chipani chanji yet munthuyo mukuti ndiwa UTM pamabvuta pati kunena zokuti akaimila UTM izo ndizachidziwikile kuti akulu amenewa UTM anaituluka kumangotsala kuti officially alengedze kuti atuluka
@EsnartMartin
4 күн бұрын
Ineso Manganya simnamulandire ku UTM
@chrispinechirwa2655
3 күн бұрын
Choyamba tidziwe kuti mu zipanimu utsogoleri umasankhidwa through convention nde kusankhidwa kwa usi sikutanthauza kuti ndi mtsogoleri wa utm. By the way the government could write aletter to utm based on their agreement to prove that the alliance is still valid. Koma kungotenga munthu personally uuùuuu it's clear usi si wa utm
@user-je8jm5uy1q
5 күн бұрын
Manganya sanali wa UTM analowa MCP kale kale mosadziwa anthu mumtima mwake anali wa MCP
@RoseLameck-ub7sq
4 күн бұрын
Ine dakalila malilo achilima singakambe kathu ndingodikila chaka chamawa ka vote bas chiweluzo nkaweluzila komweko ndichala changa😢
@Happy-e8d
4 күн бұрын
Ndinakakhala ine ndikanaka kukhala VP
@ChisomoPound
5 күн бұрын
Khaniyi mutati muyione ndiyovutirapo vuto Lili APA anthu ambiri andale amafuna maudindo ngat awa ndiye pamakhala kuyang'anizana ndi diso lofila ngat iweyo sunasakhidwe,choti muziwe Pali zina zimachitika mwamalamulo tiyeni tibwelere mbuyo 2012 bingu wa muthalika atamwalira Ku dpp kunali ambiri amafuna udindo koma anayiwala kut Kuli lamulo lot ngat president watisiya vice ndi yemwe akuyenera kukhala mlowa mmalo ndiye izizi zomwe zikuchitikazi khani siyina ayi maudindo amenewa Kuli kapezedwe Ka ndalama mwaulesi
@KhonzoBlose-wq7zm
4 күн бұрын
Move yonse yakuphedwa kwa Chilma amayiziwa asapuse fans.
@StewartMustafa
4 күн бұрын
Gentlemen plzzz lets take this issue very seriously. Dr Usi z not wrong kulandila udindo kapena kuti VP. Ndizoona kuti Dr Usi anayamba kukhala ndi boma more especially president of the republic kalekale komano chomwe tingadziwe ndichakuti even The laye Dr Saulos Chilima adali pafupi ndi boma more especially to the President of the Republic. Now gents if u digest all of these it means these pple r wel organised coz they both take one step at a time. Now lets not talk a lot of things when its not time to do so. Time will tell whereby will will proof Dr Usi that is a member of MCP or He z still with us in Almighty UTM.
@humphreysidie4747
5 күн бұрын
Guys ineso ndufuna kumangidwa, this Usi guy knew everything, he sold Chilima
@user-sh6gi5uq3l
5 күн бұрын
Akapusa a UTM a muluza manganyawo atuluka
@wellosmbewe6820
4 күн бұрын
Who is the president of UTM now and what is his speach
@user-ux3ed3ni1p
5 күн бұрын
Malamulo are there but we pick and choose what to enforce in Malawi" s constitution.
@gracemkandawire8769
5 күн бұрын
It can stay kufika pa 2 July ndipo panakhala popanda vice Kwa chaka bwa a Chilima atamangidwa
@gwatandingo9502
5 күн бұрын
Dziko La malawa amipingo ndamene anasokoneza ndi athila kuwili amasokoneza athu iwo ananena sakhani tsogoleri asakha akubweraso mwasakha thawi yolakwika kkkk koma guys mavuto Eni Eni and manganya anali wachiwili kwa wachiwili anayenera akhala iye kaya😢
@AllaniWilesi
4 күн бұрын
Ausi achita bwino inde koma asamanyengane nda azimayi ayeni pakuti Ali ndimbili yonyasa kwambili
The appointment is right decisions but there is some issues between Dr Usi and UTM party Dr Usi was not royal to the party
@laurentbutao4084
5 күн бұрын
Exactly
@KhonzoBlose-wq7zm
4 күн бұрын
Manganya he is a snake ndiwa Mcp .every knows about that, chitsilu cha munthu
@yasitafuphiri-nw2he
5 күн бұрын
If Usi was never a UTM member, y Chilima appointed him as party VP?
@jelsonmlowoka8611
5 күн бұрын
Your question is very straight and correct
@HellenKanyemba
5 күн бұрын
Atolankhani thawing zina ndinu anthira kuwili achakwera sanamusankhe usi koma achilima ndio anasankha a usi koma achakwera angitsatira lamulo basi
@user-sh6gi5uq3l
5 күн бұрын
Amalawi let's move on zinazi tichedwa nazo mulungu salakwisa kodi amalawi mpaka liti tijusungabe mangawa look at APM for not accepting the fact someone is ruling now aaaa moti a UTM amafuna kufunsidwa maganizo pomwe thawi yochita appoint veep itakwana and azichedwa ndizosangala munthu mmmmmm. Malawi my country learn to accept God's plan
@OmexPoisonkaombe-cf7bz
5 күн бұрын
Kusapanda nseru anapha bwanji vice president wathu ameneyo bas
@williamsjonazie5764
5 күн бұрын
Choyamba tiwunikile Kaye kuti Kodi chakwera poziwa kuti usi ndi vice president wa UTM anawawuza za appointment ya usi? Ngati adatelo ndiye a UTM analakwisa kusapita koma ngati sadawauze za kusakhidwa Kwa usi adachita bwino kusapita chifukwa usi wangokhala vice president wa UTM koma ndi member wa UTM,executive ikanaziwisidwa mwa dongosolo and then invited kukalumbilitsa vice president. Nde anthu musamangofutsa mafutso mwina mufutse chakwera yo. Ndamene angalongosole momwe adayendesela ndondomeko yake.
@MarkGonda-qr4vm
3 күн бұрын
Koma ndiye azingopanga zamasewerotu amanganyawa
@user-ql8sj4jj3y
4 күн бұрын
Manganya ndi mcp,, if he was vice wa chilima, atamwalira dr chilima was just qite why
@user-eb2yo9bc9k
5 күн бұрын
I doubt of all this, am confused but what I know is that utm is not happy with that
@Shire9627
5 күн бұрын
Malawians timadana ndi chilungamo🤣🤣🤣
@isaihmagani5697
5 күн бұрын
A UTM ku sapita kolumbilitsa a Usi nkutheka sadalakwise mwina sadayitanidwe patha kukhara padalibe consultations,
@user-vm7iz6oz6r
5 күн бұрын
Awusi anarephera kutengapo gawo, kufa kwa skc relo palibe sngakondwe nazo asiyen azipanga zomwe amatha ndi kongweresi yakeyo
@JackMvura-ik2td
5 күн бұрын
Munena angati mutukwana angati anzathu patsogolo Ife basi zaziii nthawi ikupita tichedwa zinenani bola chakwera sadandaula anaona kale Kuti sanje zilipo kuteloku Wena mtima uwawa Kuti basi manganya wapita basi ayi zosiyilana mawa ndinu pepani mulungu akusungeni
@RonaldGama-gz9ug
5 күн бұрын
Kodi a UTM wo mukuwafuna kuti atanipo Pa nkhaniyi coz they can't reserve the time anayankha zomwe iwo Ali ndiye chinanso ndi chani
@TaniaMphalumo
5 күн бұрын
Zauchisilu basi wasangalalanazo ndani utm muyisiye agaru inu
@user-ql8sj4jj3y
4 күн бұрын
Total lay dpp sizikuwakhuza
@Stewartchikoja
5 күн бұрын
Kodi ngat wina adakhala Dzaka 4 osapenza mpumulo pa office yake how about 1 Yr chingasithe ndi chani ?
@VictoriaWilliam-ms2ft
5 күн бұрын
Usi siwa utm ndiwa mcp uja musatinamizepo apa
@MCAnthonyNdau
5 күн бұрын
Ndichimodzi modzi bingu atamwalila sitinakhale ndi pulezident wanyowani
@MayiSwale
5 күн бұрын
Chanzeru ndi chani??? Zaziiii
@sarahmphande6108
2 күн бұрын
It not alaw, kut you must choose the vice president wachipani, that is a trap iwe manganya akupasa zingati why you didn't have time to settle and see it with your utm people
Utsi nd wa mcp inu a utm mukapusa mugulitsa chipan😮
@Maliet-nh6kf
4 күн бұрын
But why you killing others skc he made mcp to be on position later on decide 😈 chakwera pathako pako malo mobweza ulem ndikupha munthu😢😢😢
@princedetbozsmallboy1749
5 күн бұрын
Inuyoso nanu aaàa manganyayu anapha nawo Chilima galu wamunthu uyu kakuwoneka mumask ka manganyaka kanachenjela udyo
@EstherAmadu-md3et
5 күн бұрын
Koma abale manganya angakhale wachiwiri wa ntsogoleri wa dziko mmmm dziko limafuna kutsogoleledwa ndi anthu a serious uyu anthu sangamunvele akapitilize ma drama
@KenDuweh
5 күн бұрын
Muwawudze a Micheal usi kuti watikumbutsa za mbala ziwiri pa mtanda ifeo timukumbutse za Yudas isikaliyot uja unapeleka Yesu khristu kuti kodzi zinankhla bwanji? Zandale tiyen tizingoona😅
@user-pv9uk6sc3w
5 күн бұрын
Palibe chimene angachite Usi, and Malemu ndiamene adatsogolera kubweretsa mavuto ali ku Malawi lero.
@user-ui7wv1mb4g
5 күн бұрын
What mavuto are you talking about . Was he on the driving seat? Kufooka kwa wina osaloza chala ena
@kamphunguluhanga5716
5 күн бұрын
Osagwirizana nazozo akulakwa. Chifukwa or vhikqnkhala kuti running mate akanakhala Rasta Chikomeni zikanakhala momwemo basi. Munthu uyu wotchedwa Chakwera ndi Munthu woyenera usogoleri. Chifukwa watsata ndondomeko yamugwirizano wawo komnso kutsatira constitution ya Presidencey
@user-mm9ox2pz7p
5 күн бұрын
Zaziiiii mwasowa zokambirana
@TsholofeloTong
5 күн бұрын
Usi please just go to your MCP because we already know that you're mcp member
Пікірлер: 153